Publicidade

Jeremias 6

16 Yehova akuti,

"Imani pa mphambano ndipo mupenye;

kumeneko ndiye kuli njira zakale,

funsani kumene kuli njira yabwino. Yendani mʼmenemo,

ndipo mudzapeza mpumulo wa miyoyo yanu.

Koma inu munati, Ife sitidzayenda njira imeneyo.

Veja também

Publicidade
Bíblia Online Bíblia Online

Bíblia Online • Versão: 2026-06-29_22-07-56-