10 Usasiye bwenzi lako ndiponso bwenzi la abambo ako,
ndipo usapite ku nyumba ya mʼbale wako pamene wakumana ndi mavuto;
mnzako wokhala naye pafupi amaposa mʼbale wako wokhala kutali.
10 Usasiye bwenzi lako ndiponso bwenzi la abambo ako,
ndipo usapite ku nyumba ya mʼbale wako pamene wakumana ndi mavuto;
mnzako wokhala naye pafupi amaposa mʼbale wako wokhala kutali.