10 Milagres de Jesus na Bíblia: Lista com versículos e explicação
Os milagres de Jesus são muito mais do que demonstrações de poder sobrenatural; eles são sinais que confirmam sua divindade e missão. Ao longo dos Evangelhos, vemos Cristo curando enfermos, dominando a natureza e vencendo a morte.
Neste guia, selecionamos 10 milagres de Jesus na Bíblia, organizados com referências e uma breve explicação sobre o impacto espiritual de cada um deles.
Os principais milagres de Jesus nos Evangelhos
1. Transformação da Água em Vinho
Referência: João 2:1-11
Explicação: Ocorreu nas Bodas de Caná. Sendo o seu primeiro milagre público, Jesus demonstrou autoridade sobre a matéria e a natureza, revelando sua glória aos discípulos e abençoando a instituição da família.
Ukwati mmujhi wa Kana
Siku la katatu kudali ni ukwati mmujhi wa Kana, mkoa wa ku Galilaya, nawo amaye wake Yesu adalipo pamwepo, Yesu naye wadalalikidwa pa ukwati pamojhi ni oyaluzidwa wake. Divai yapo idatha, amaye wake adamkambila Yesu, "Divai yatha."
Ndiipo Yesu wadayangha amaye wake, "Ndandeyanji munikambila nghani imeneyo. Ndhawi yochita njhito yanga ikali yosafika."
Chimwecho amake adazikambila mbowa, "Chilichonjhe icho siwakukambileni, chitani,"
Pamenepo padali ni mapipa sita ya myala, iyo yaikidwa kwa chikhalidwe chakusamba cha Chiyahudi, kila mchuko udakakhoza kutenga michuko ya wili kapina itatu ya majhi. Ndiipo Yesu wadaakambila, "Jhazani majhi mmapipa." Ndiipo wadaakambilanjho, "Chipano tungani mkampelekele wamkulu wa phwando." Wamkulu waphwando yapo wadalawa majhi yameneyo, wadapeza yang’anamuka kukhala divai. Siwada jhiwe uko ya choka, nambho anyiyawo adatunga majhi adajhiwa. Wamkulu wa phwando wadamtana wammuna wa ukwati, wadamkambila, "Kila mudhu wayamba kwapacha wandhu divai ya bwino uti, ni akathokumwa ni kukwana, wakonja ijha yosakome. Nambho iwe wachocha divai ya bwino mbaka saino."
Yesu wadachita chizindikilo ichi choyamba ku Kana, ya ku Galilaya wadaalangiza ulemelelo wake, ni oyaluzidwa wake adamkhulupilila.
2. Cura do cego de nascença
Referência: João 9:1-12
Explicação: Jesus usa lodo para curar um homem que nunca havia enxergado. Este milagre prova que Ele é a Luz do Mundo e tem poder para restaurar o que nasceu com defeito.
Yesu wamlamicha mundhu uyo wabadwa osapenya
Siku limojhi Yesu yapo wamapita wadamuona mundhu mmojhi, uyo siwapenya kuyambila kubadwa kwake. Basi oyaluzidwa wake adamfunjha, "Oyaluza! Yani wachita machimo, mundhu uyu kapina obala wake, mbaka wabadwe osapenye?"
Yesu wadaayangha, "Wabadwa osapenye osati ndande ya machimo yake, kapina ya obala wake, wadabadwa chimwecho kuti mbhavu ya Amnungu iwoneke muumoyo wake. Ifunika tiendekele kuzichita njhito za yawo atituma kukali usana, ndande usiku ukujha uwo mundhu waliyonjhe siwakhoza kuchita njhito. Ndhawi nili pano pajhiko, ine nde dangalila la wandhu a pajhiko."
Yapo wadakamba chimwecho, wadalavula malovu panjhi, wadakonja thokope, wadamnyeka yujha osapenyeyo mmaso, wadamkambila, "Pita ukasambe kuthiwi la Siloamu." Mawu Siloamu mate yake Uyo watumidwa. Chimwecho wadapita kusamba, wadabwela uku ni wapenya.
Ndiipo, apafupi wake ni wina yao amajhiwa kuti poyamba wadali osauka pembhapembha, adakamba, "Uyu osati osauka yujha wamakhala ni kupembha?"
Wina adakamba, "Ndemwene." Wina adakambanjho, "Notho! Wangolingana nayo."
Nambho yujha wadali osapenyayo wadakamba, "Nde ine!"
Basi amamfunjha, "Chipano, maso yako yakhoza bwanji kupenya?"
Wadayangha, "Yujha mundu watanidwa Yesu wadakonja thokope, wadaninyeka mmaso ni kunikambila nipite nikasambe ku thiwi la Siloamu. Pamenepo ine nidapita kusamba kumaso, pampajha nidakhoza kupenya."
Adamfunjha, "Iye walikuti?" Nayo wadaayangha,
"Ine sinijhiwa!"
3. Multiplicação dos pães e peixes
Referência: Mateus 14:13-21
Explicação: Com apenas cinco pães e dois peixes, Jesus alimentou mais de 5 mil homens. Este sinal revela Cristo como o Pão da Vida, aquele que supre todas as nossas necessidades.
Yesu waaningha chakudya wandhu kupitilila elfu zisano
Yesu yapo wadavela nghani za Yohana, wadachoka malo yajha kwa boti, wadapita pamalo popande wandhu kuti wakhale yokha. Nambho wandhu yapo adavela adamchata poyenda pa mwendo kuchokela mmijhi yao. Yesu yapo wadachika mboti, wadaliona gulu lalikulu la wandhu, wadaonela lisungu ni wadaalamicha odwala wao.
Ujhulo yapo udafika, oyaluzidwa wake adamchata ni kumkambila, "Malo yano ni paphululu, jhuwa litobila. Walole wandhu apite kumijhi akajhigulile chakudya."
Yesu wadaakambila, "Siifunika achoke, anyiimwe mwachinawene wake mwaapache chakudya."
Anyiiwo adamuyangha, "Tulinayo mabumunda isanope ni njhomba ziwili."
Yesu wadaakambila, "Nipelekeleni pano." Wadaakambila wandhu akhale mmaujhu. Yesu wadatenga mabumunda yasano ni njhombha ziwili zijha, wadakweza maso yake kumwamba, wadamyamika Mnungu. Halafu wadabandhula mabumunda ni kwaapacha oyaluzidwa wake, naonjho oyaluzidwa wake wadaagawila wandhu. Wandhu wonjhe adadya ni kukhuta. Oyaluzidwa adakokola vidufya ivo vidakhalila ni kujhaza miseche khumi ni iwili. Wachimuna yawo adadya adali ngati elufu zisano, nambho waachikazi ni wana siadawelengedwe.
4. Jesus acalma a tempestade
Referência: Marcos 4:35-41
Explicação: Com uma ordem, o vento e o mar se aquietam. O milagre ensina sobre a paz que excede o entendimento e a autoridade do Messias sobre a criação.
Yesu waunyindila mwela
Siku limwelo ujhulo, Yesu wadaakambila oyaluzidwa wake, "Tiyomboke chijya la nyanja Galilaya." Adausiya ujha msonghano wa wandhu, oyaluzidwa adapita pamojhi ni iye mboti mujha wadalimo Yesu, adachoka nayo. Chimwechonjo kudali ni maboti ina yambili pamalo pamenepo. Papajha mwela waukulu udachokela, ni mafunde yadalibula lijha boti wadalimo Yesu mbaka lidayamba kujhala majhi. Yesu wadali kumbuyo kwa lijha boti wadatogonela philo, oyaluzidwa wake adamuucha ni kumkambila, "Oyaluza, simganizila kuti ife titobila?"
Ndiipo Yesu wadauka ni kuunyindila mwela, "Khala chete!" Pampajha mwela udasiya ni nyanja idagona.
Chimwecho Yesu wadaakambila oyaluzidwa wake, "Ndande yanji muopa? Bwanji, mkali mlibe chikulupililo?"
Oyaluzidwa wake adaopa kupunda, adafunjhana, "Mundhu wa mtundu wanji uyu mbaka mwela umvela?"
5. Cura da mulher com fluxo de sangue
Referência: Marcos 5:25-34
Explicação: Uma cura que aconteceu pelo toque da fé. Jesus mostra que está atento ao sofrimento individual e que a fé é o canal para receber o milagre.
Pajha pagulu wadalipo ni wamkazi uyo wamadwala utenda wosusa nghole kwa vyaka khumi ni viwili. Wamkazi mmeneyo wadavutika kupunda kwakupita kwa asing’anga ambili ni wadatumia chuma chake chonjhe, nambho siwadalame, ni wadaendendekela kudwala kupunda. Wamkazi yujha yapo wadavela nghani za Yesu, wadapekenyela paghulu la wandhu, wadampitila Yesu kwa kumbuyo ni kugafya njhalu yake. Wadajhikambila mumtima mwake, "Nikagafyape njhalu yake, sinilame." Yapo wadagafyape njhalu ya Yesu, pampajha nghole idasiya kususa, nayo wadajhivela thupi lake lalamilatu.
Pampajha Yesu wadajhiwa kuti mbhavu zake zolamicha zatumika, chimwecho wadaling’anamukila lijha gulu la wandhu ni kufunjha, "Bwanji, yani uyo wagafya njhalu yanga?" Oyaluzidwa wake adamuyangha, "Uona umo wandhu akubwanyizilabwanyizila, chipano ufunjha bwanji kuti yani wakugafya?" Nambho Yesu wadayendekela kupenya kuti wamuone uyo wamgafya. Wamkazi mmeneyo wadajhiwa yayo yadachitika kwa iye, chimwecho wadampitila Yesu uku ni watendhemela kwa mandha. Wadagwada pachogolo pa Yesu ni kumkambila uzene wonjhe. Yesu wadamkambila, "Mwali, chikhulupililo chako chakulamicha. Pita kwa mtendele, walama utenda wako."
6. Libertação do endemoninhado Gadareno
Referência: Marcos 5:1-20
Explicação: Jesus liberta um homem dominado por uma legião de espíritos. É a prova clara de sua autoridade absoluta sobre o reino das trevas.
Yesu wamlamicha mundhu wa viwanda vambili
Yesu ni oyaluzidwa wake adafika kuchijya kwa nyanja ya Galilaya mjhiko la Agelasi. Yesu yapo wadandochikape mboti, wadapezana ni mundhu uyo wadali ni chiwanda, mundhu mmeneyo wamachokela kumainja. Mundhu mmeneyo wamakhala kujha kumainja, ni palibe mundhu wamakhoza kummanga ata kwa maunyolo. Pakuti mala zambili amammanga maunyolo mmanja ni phingu mnywendo, nambho wamadula yajha maunyolo ni kuzidula zijha phingu myendo yake. Wadali ni nghongono zambili, ni padalibe mundhu waliyonjhe wamakoza kumgwila. Usana ni usiku kuzungulila kumainja ni kuphili, niwabula pokoso ni kujhiduladula kwa myala.
Yapo wadamuona Yesu kwa kutali, wadamthamangila, ni kumgwadila. Ni wadakekema kwa mvekelo wa ukulu, "Ufuna kunichita chiyani iwe Yesu Mwana wa Mnungu wali kumwamba kupunda? Nikupembha kwa jhina la Mnungu siudani vuticha!" Wadakamba chimwecho pakuti Yesu wadachikambila, "Chiwanda, choka kwa mundhu uyu"
Ndiipo, Yesu wadachifunjha, "Jhina lako yani"
Wadamuyangha, "Jhina langa ni gulu pakuti tili tambili." Ndiipo adampembha kupunda Yesu wasavitopola vijha viwanda ni kuvipeleka kubwalo kwajhiko lijha. Pafupi ni pamenepo lidalipo gulu lalikulu la nguluwe nilidya pafupi ni phili. Chimwecho vijha viwanda vidampembha Yesu, "Utipeleke kwa nguluwe, utisiye tizilowe izo." Ndiipo Yesu wadavivomeleza, ni vijha viwanda vidamchoka mundhu yujha ni kulowa kwa nguluwe. Gulu lonjhe la nguluwe, zidachikilila kumchikililo ni kubila mmajhi ni kufa, zidali nguluwe alufu ziwili.
Anyiwajha amasunga nguluwe adathamanga, kupita kuvijhijhi ni kuminda kwakambila wandhu yameneyo yadachokela. Wandhu wonjhe adapita kuona yajha yadachokela. Yapo adafika kwa Yesu, adamwona yujha mundhu wadazamwa ni viwanda vambili wakhala panjhi, uku wavala njhalu zonjhe, wali wolungwamika, ni wandhu wonjhe adaopa. Wandhu wajha adaona vindhu vimenevo, adaakambila wandhu wina vindhu ivo vidamchokela yujha mundhu wadali ni viwanda ni lijha gulu la nguluwe. Ndiipo, wandhu adampembha kupunda Yesu wachoke mjhiko mwao. Ndiipo Yesu yapo wamakwela mboti, yujha mundhu wadachochedwa viwanda wadampembha Yesu apite wonjhe. Yesu siwadamvomeleze, wadamkambila, "Pita kukhomo kwa achaabale wako ukakambile vindhu vavikulu ivo akuchitila Ambuye Mnungu, ni umo adakulengela lisungu." Chimwecho yujha mundhu wadachoka ni kupita kuuzila ku Dekapoli mate yake mijhi khumi vindhu ivo Yesu wadamchitila, ni wandhu wonjhe adazizwa.
7. Ressurreição da filha de Jairo
Referência: Marcos 5:21-43
Explicação: Jesus demonstra que a morte para Ele é como o sono. Ele restaura a vida de uma criança, trazendo esperança para uma família desesperada.
Yesu wamuhyukicha Mwali wa Yailo ni kumlamicha wamkazi
Yesu yapo wadayombokanjho kwa boti ni kufika kuchijya. Gulu lalikulu la wandhu lidamzungulila, iye wadaima mbhepete mwa nyanja. Mmojhi wa achogoleli anyumba yokomanilana Ayahudi uyo wamatanidwa Yailo wadajha pamenepo, niiye yapo wadamwona Yesu wadamgwadila, wadampemba niwakamba, "Mwali wanga wadwala pafupi kumwalila. Chonde nikupembha majha umuikile manja nawo wakhoze kulama ni kukhala wamoyo." Chimwecho Yesu wadapita pamojhi niiye. Ni gulu lalukulu la wandhu limamchata, uku ni niabwanyizabwanyiza. Pajha pagulu wadalipo ni wamkazi uyo wamadwala utenda wosusa nghole kwa vyaka khumi ni viwili. Wamkazi mmeneyo wadavutika kupunda kwakupita kwa asing’anga ambili ni wadatumia chuma chake chonjhe, nambho siwadalame, ni wadaendendekela kudwala kupunda. Wamkazi yujha yapo wadavela nghani za Yesu, wadapekenyela paghulu la wandhu, wadampitila Yesu kwa kumbuyo ni kugafya njhalu yake. Wadajhikambila mumtima mwake, "Nikagafyape njhalu yake, sinilame." Yapo wadagafyape njhalu ya Yesu, pampajha nghole idasiya kususa, nayo wadajhivela thupi lake lalamilatu.
Pampajha Yesu wadajhiwa kuti mbhavu zake zolamicha zatumika, chimwecho wadaling’anamukila lijha gulu la wandhu ni kufunjha, "Bwanji, yani uyo wagafya njhalu yanga?" Oyaluzidwa wake adamuyangha, "Uona umo wandhu akubwanyizilabwanyizila, chipano ufunjha bwanji kuti yani wakugafya?" Nambho Yesu wadayendekela kupenya kuti wamuone uyo wamgafya. Wamkazi mmeneyo wadajhiwa yayo yadachitika kwa iye, chimwecho wadampitila Yesu uku ni watendhemela kwa mandha. Wadagwada pachogolo pa Yesu ni kumkambila uzene wonjhe. Yesu wadamkambila, "Mwali, chikhulupililo chako chakulamicha. Pita kwa mtendele, walama utenda wako."
Yesu yapo wamaendekela kukamba, wandhu wina adajha kuchokela kwa Yailo, ni adamkambila, "Mwali wako wathomwalila, ndande yanji uyendekela kwaachaucha oyaluza?" Nambho, Yesu yapo wadavela chindhu chijha adachikamba, siwadalitengele mate, wadamkambila yujha wamkulu wa nyumba yokomanilana, "Siudaopa, iwe khulupililape." Ndiipo Yesu siwadafune mundhu waliyonjhe wamchate, nambho wadapita ni Petulo, ni Yakobo ni Yohana mphwake wa Yakobo.
Yapo adafika kukhomo kwa Yailo, Yesu wamavela mapokoso ni vililo. Yesu wadalowa mkati, wadaafunjha "Bwanji mbula pokoso ni kulila? Mwana siwadamwalile, nambho wagonape." Nambho wandhu wajha adamseka. Chimwecho wadaachocha kubwalo, wadaatenga atate ni amake wa yujha mwali, ni wajha oyaluzidwa wake yawo wadali nawo, adalowa kuchumba chijha adagoneka chitanda chayujha mwali. Yesu wadamgwila jhanja, wadamkambila, "Talisa khumi!" Mate yake, "Mwali, nikukambila uka!" Pampajha yujha mwali wadaima, ni kuyamba kuyenda, mwali yujha wadali ni vyaka khumi ni viwili. Chindhu chimenecho yapo chidachokela, obala ni wajha oyaluzidwa adalowa mujha adazizwa kupunda. Yesu wadaakaniza kupunda siadamkambila mundhu waliyonjhe chindhu icho chidachokela. Ndiipo wadaakambila obala wake, "Mpacheni mwali chakudya kuti wadye."
8. Jesus anda sobre as águas
Referência: Mateus 14:22-33
Explicação: Ao caminhar sobre o Mar da Galileia, Jesus mostra que não está sujeito às leis da física. O episódio também serve para tratar a fé e a dúvida no coração de Pedro.
Yesu wayenda pa mwamba pa majhi
Yesu yapo wamalaila wandhu, wadaakambila oyaluzidwa wake akwele mbwato wa ukulu kuti achogolele kupita kuchijya kwa nyanja ya Galilaya. Yapo wadamaliza kwalaila wandhu, wadakwela kuphili kukapembhela. Wadakhala kumeneko yokha mbaka usiku yapo udajha. Ndhawi imeneyo bwato lalikulu lidafika pakatikati pa nyanja, uku nilindengandenga kwa mafunde ndande mbhepo imalibula.
Mmalenga kucha, Yesu wadaachata oyaluzidwa uku niwayenda pa mwamba pa majhi. Oyaluzidwa wake yapo adamwona niwayenda pa mwamba pa majhi, adaopa ni kukamba, "Chimzilimu!" Adabula phokoso ndande ya mandha.
Nambho pampajha Yesu wadaakambila, "Jhithileni mtima, ni ine. Msadaopa!"
Petulo wadamkambila, "Ambuye, ngati nde imwe, nikambileni nikuchateni pakuyenda pa mwamba pa majhi."
Yesu wadamkambila, "Chabwino, majha." Ndiipo Petulo wadachika mbwato waukulu, wadayenda pamwamba pa majhi ni kumpitila Yesu. Petulo yapo wadawona mbhepo yaikulu, wadaopa ni kuyamba kubila uku niwabula phokoso, "Ambuye, nipulumucheni!"
Pampajha, Yesu wadatambasula jhanja lake, wadamgwila ni kumkambila, "Iwe wa chikulupi chochepa, ndande yanji uopa?"
Ndiipo adakwela mbwato waukulu, ni mbhepo nayonjho idasiya. Wonjhe adali mbwato waukulu, adagwada ni kumkwatamila, niakamba, "Zenedi iwe ni Mwana wa Mnungu."
9. Cura do paralítico
Referência: Marcos 2:1-12
Explicação: Jesus cura o corpo, mas primeiro perdoa os pecados. Este milagre estabelece que sua missão principal é a reconciliação espiritual do homem com Deus.
Yesu wamlamicha mundhu wovuwala
Yapo yadapita masiku yochepa, Yesu wadabwelanjho kumujhi wa Kapelinaumu, wandhu adavela kuti wali kukhomo. Wandhu ambili adakomana pamojhi, mbaka padalibe malo yokhala, adajhala pa liwala pa nyumba. Yesu wamalalikila uthenga wa Mnungu. Pamenepo, adafika wandhu anayi, adamtenga mundhu wovuwala, adampeleka kwa Yesu. Saadakhoze kumpeleka pafupi ni Yesu ndande ya lijha gulu la wandhu. Chimwecho adakwela pamwamba, adafulumula chindu, pajha wadali Yesu. Yapo adafulumula, adamchicha mundhu yujha uku amgoneka pa chitala. Yesu yapo wadaona chikhulupililo chao, wadamkambila yujha mundhu wovuwala, "Bwenji langa, nakulekelela machimo yako." Woyaluza akumojhi athauko la Musa, yawo adali pamenepo adaganizila mmitima yao, "Chindhu chanji icho chimkhozecha kukamba chimwechi? Wamkafula Mnungu! Ni Mnungu yokha uyo wakhoza kulekelela machimo." Pampajha, Yesu wadayajhiwa yayo amaganizila mmitima yao, wadaakambila, "Bwanji mganiza chimwecho? Nichiti chili chopepuka kupunda, kumkambila mundhu uyu wavuwala, ‘Walekeledwa machimo yako,’ kapina kumkambila, ‘Uka, utenge chitala chako upite?’ Chipano, nifuna mjhiwe kuti ine Mwana wa Mundhu nali ni ulamulilo wolekelela machimo ya wandhu pajhiko." Pamenepo, wadamkambila yujha mundhu wadavuwala, "Nikukambila, uka utenge chitala chako, upite kukhomo!"
Pampajha yujha wodwala wadauka, wadatenga chitala chake ni kuchoka, uku wandhu wonjhe niampenya. Wandhu wonjhe adazizwa ni kumtamanda Mnungu, niakamba, "Sitidaonepo chindhu ngati ichi."
10. Ressurreição de Lázaro
Referência: João 11:1-44
Explicação: O milagre mais impactante antes da crucificação. Ao ressuscitar alguém morto há quatro dias, Jesus declara: "Eu sou a ressurreição e a vida".
Kumwalila kwa Lazalo
Padali ni mundhu mmojhi wa ku Besania, wamatanidwa Lazalo, wamadwala. Wamakhala kuchijhijhi cha Besania kumeneko amakhala ni achalongo wake Malia ni Masa. Malia uyu nde yujha wadaanyeka Ambuye mafuta ya mtengo wa ukulu yayo yanunghila ni kuichangula myendo kwa machichi yake. Mbale wake Lazalo nde uyo wadali odwala. Chimwecho achalongo wake Lazalo onjhe adatuma uthenga kwa Yesu, "Ambuye mmbwenji lanu wadwala!"
Yesu yapo wadavela chimwecho, wadakamba, "Lazalo siwamwalila kwa utenda uno, nambho wadwala ndande ya kwaapacha Amnungu ulemelelo, wadwala dala Mwana wa Amnungu walemekezedwe kupitila utenda umeneo."
Yesu wadali ni ubwenji wa pamtima ni Masa ni Malia ni Lazalo. Yapo wadavela kuti Lazalo wadwala, Yesu wadaendekela kukhala pamalo pajha wadali kwa masiku yawili. Ndiipo pambuyo pa yameneyo, wadakambila oyaluzidwa wake, "Chipano tiyeni tibwelenjho ku Yudea!"
Oyaluzidwa wake adamkambila, "Oyaluza! Yapita ndhawi yo chepa Ayahudi yapo amafuna kuiiphani kwa myala, ndande yanji mfuna kupitanjho kumeneko?"
Yesu wadayangha, "Bwanji saa za usana osati khumi ni ziwili? Chimwecho mundhu akayenda usana siakhoza kujhikhuwala ndande aliona dangalila la jhiko lino. Nambho usiku mundhu wajhikwala ndande dangalila palibemo mkati mwake." Yesu yapo wadakamba mawu yameneyo, wadaakambila, "Mbwenji lathu Lazalo waghona litulo, nambho ine sinipite kumuucha."
Oyaluzidwa wake adamkaambila, "Ambuye ngati waghona, siwauke."
Anyiiwo amaghaniza wamakamba kuti waghona litulo, nambho wamakambilila nyifa ya Lazalo. Ndiipo, Yesu wadakambila popande kwa bisa, "Lazalo wamwalila, nambho nikondwa ndande sinidalipo kumenepo yapo Lazalo wamamwalila. Chipano tiyeni kukhomo lake."
Tomaso uyo watanidwa mawila wadaakambila oyaluzidwa achanjake kuti, "Tiyeni nafe tikafe pamojhi ni Ambuye!"
Yesu nde uhyucho ni umoyo
Yesu yapo wadajha kumeneko wadapheza chitanda cha Lazalo chatho khala siku zinayi mmainja. Kijhijhi cha Besania chidali pafupi ni Yelusalemu, utali wa kilometa zitatu kuchoka ku Yelusalemu. Ayahudi ambili adafika kwa masa ni Malia kwa tondeza kwa nyifa ya mlongo wao.
Chimwecho Masa yapo wadavela kuti Yesu watokujha, wadapita kumlandila nambho Malia wadakhala pakhomo. Ndiipo Masa wadamkambila Yesu, "Ambuye, ngati mudakalipo pano, mlongo wanga siwadakafa! Nambho nijhiwa kuti atangati chipano chilichonjhe icho siwapembhe Amnungu, sakupacheni."
Ndiipo Yesu wadamkambila, "Mlongo wako siwahyuke."
Masa wadayangha, "Nijhiwa kuti siwahyuke ndhawi ya uhyucho, siku lo thela."
Yesu wadamkambila, "Ine nde uhyucho ni umoyo. Uyo wanikhulupilila ine atangati wakamwalila, siwakhale moyo, ni waliyonjhe uyo wakhala wa moyo ni khulupilila, siwamwalila muyaya. Bwanji ulikhulupilila ili?"
Masa wadamkambila, "Etu Ambuye! Ine nikhulupila kuti imwe nde Kilisito uyo wasanghidwa ni Amnungu, Mwana wa Amnungu, uyo wakujha pajhiko."
Yesu wamlilila Lazalo
Pambuyo pa yameneyo, Masa wadapita kumtana Malia kwa chisisi, wadamkambila, "Oyaluza alipano, akutanani." Nayo yapo wadavela chimwecho wadaima msangu, ni kumchata Yesu. Ni Yesu wadaliwakali osafike pa kijhijhi, wadali wakali pamalo pampajha wadalandilidwa ni Masa. Ndiipo Ayahudi anyiyawo adali mnyumba ni amtondeza Malia yapo adamuona mujha waima ni kutuluka kubwalo chisanga, adamchata. Amaghaniza wapita kumanda kuomboleza.
Ndiipo, Malia yapo wadafika pamalo yapo wadali Yesu, wadagwada, wadamkambila, "Ambuye, ngati mudakali pano, mlongo wanga siwadakamwalila!"
Yesu yapo wadamuona maliya walila, ni Ayahudi anyiyao adajha pamojhi ni Maliya nayo alila, wadali ni chisoni ni kudandaula mumtima. Ndiipo wadamfunjha, "Mwamzika kuti?"
Adamkambila, "Ambuye, majhani mpenye."
Yesu wadalila. Chimwecho, Ayahudi adakamba, "Penyani umo wamkondela Lazalo!"
Nambho wina adakamba, "Uyu wadalamicha maso yujha sapenya, siwadakhoza kumlamicha Lazalo?"
Yesu wamuhyucha Lazalo
Ndiipo Yesu uku ni wadandaula mumtima, wadafika yapo idali manda. Manda ene idali mbhanga, ni ida vinikilidwa mwala. Yesu wadakamba, "Uchocheni mwala!" Masa mlongo wake Lazalo, wadamkambila, "Ambuye, watho yamba kunungha, ndande wakhala mmanda siku zinai!"
Yesu wadaamkambila Masa, "Bwanji sinidakukambileni kuti ukakhulupilila siuone ulemelelo wa Amnungu?" Ndiipo adauchocha ujha mwala. Yesu wadapenya kumwamba, wapemba, ni wakamba "Nikuyamikani Atate ndande mwanivela. Nijhiwa kuti munivela siku zonjhe. Nakamba yameneyo ndande ya wandhu alipano kuti apheze kukhulupilila kuti imwe nde yao mwanituma." Yapo wadamaliza kukamba yameneyo, wadatana kwa mvekelo waukulu, "Lazalo, majha kuno kubwalo!" Yujha wadamwalila wadatuluka kubwalo, wali omangidwa sanda mmyendo ni mmanja, ni kumaso wavinikilidwa njhalu.
Yesu wadakambila, "Mmasuleni, mumsiye wajhipita."
Conclusão
Os milagres de Jesus revelam sua autoridade sobre a natureza, as enfermidades, o mundo espiritual e até a morte. Eles não são apenas demonstrações de poder, mas sinais que apontam para sua identidade e missão.
Ao estudar esses milagres, é possível compreender melhor o papel de Jesus e a mensagem central do Evangelho.
Se este conteúdo ajudou você a entender os milagres de Jesus na Bíblia, compartilhe este artigo para que mais pessoas também conheçam esses ensinamentos.