1 Nchimwecho abale wanga, nikukondani nikhumbila kupunda kukuonani anyiimwe muli chikondi changa ni mbhaso yanga, chimwechi ndeumo mfunika kukhala nganganga ni Ambuye anyiimwe nikukondani.
2 Nialilila Euodia ni Sintike, nikupembhani mgwilizane ngati abale mwa Ambuye. 3 Yeetu nikupembhanjho, iwe wakulupila kwatangatila wachikazi anyiyawa ainjili pamojhi niine, Kilimenti ni atumiki anjanga winanjho, anyiyawo mayina yawo yalembedwa muchikalakala cha umoyo.
4 Chimwemwe chanu mwa Ambuye kwambili. Nikamba muchimwemwe!
5 Upole wanu ujhiwike ni wandhu onjhe. Ambuye ali pafupi. 6 Msadachita mandha pa chindhu chalichonjhe, nambho pa kila chindhu, pa kwapembha Mnungu mwa mayamiko, ni mapembhelo yanu siya jhuwike. 7 Ni mtendele wa Amnungu, upitilila njelu zonjhe, zikusungeni mitima yanu, ni njelu zanu, mwa Kilisito Yesu.
8 Potela mpenye vindhu vazene, ni yamate, yavomeleka, yaelecheka, yakhadwa ni yaulemu. 9 Vindhu vonjhe mwajiyaluza kwanga kapina kuyalandila kapina kuyavela kapina kuyaona, yachiteni yameneyo. Ni Mnungu watupacha mtendele siwakhale pamojhi nianyiimwe.
10 Nili nichimwemwe kupunda mwa Ambuye, nchimwecho mwayambanjho kunitumikla, zene mwayamba kuniganizila, nambho simudapheze kuchita chimwecho 11 Sinikamba nchimwechi ndande nifuna iyayi, pakuti nilizika kwa umo siikhalile. 12 Nijhiwa umo ikhalila pajha ukhala opande kandhu, ni ukakhala ni kandhu, najiyaluza nikhale nacho, kapina nikhale ni njala, chikhale chambili, kapina chochepekela. 13 Nikhoza kuchita vindhu vonjhe mwa iye wanipacha mbhavu.
14 Atamchimwecho, anyiimwe mwachita bwino kugwilizana mwa mavuto yanga. 15 Ata anyiimwe Afilipi mujhiwa mmayambo mwo lalikila Injili pajha nimaachoka ku Makedonia palibe wandhu okhulupilila wina adanithangatila kuusu kuchocha ni kulandila ila anyiimwe mweka. 16 Pakuti ata kujha ku Selonike mdani pacha mtandizo mala kambili. 17 Osati nikhumbila ijha mbhaso, nambho nikhumbila mbhaso ichuluke kwanu. 18 Nalandila kila kandhu, kupitila Epafulodito nambho vachulukila, nalandila kwa Epafulodito vindhu vachoka kwanu, ndalama ni Mnungu avivomela. 19 Ni Mnungu wanga siakupacheni kila icho mufuna, kwa umo ali Opata mwa ufulu, wa Kilisito Yesu. 20 Chipano wakwezedwe Mnungu ni Atate muya ni muyaya ikhale chimwecho.
21 Muni lonjelele aikidwa kwa kulalikila Uthenga Wabwino wa Kilisito. Abale ali pamojhi niine akulonjelani. 22 Ulonjeledwa ni aikidwa kwa njhito asa anyiwajha a nyumba ya chifumu ya Kaisali.
23 Mwachitilidwa ubwino wa Ambuye Yesu Kilisito pamojhi ni mzimu wanu.