O que é bom
O que é bom vem de Deus. A Bíblia celebra a bondade divina e nos convida a discernir, praticar e desfrutar tudo o que é bom — porque toda boa dádiva vem do Pai das luzes.
Chimwecho thauko lene lachoka kwa Mnungu, ni lamulo lene lachoka kwa Mnungu, ni yali ngati umo yafunikila ni yabwino
Simudaganizila ngati wandhu ajhiko lino umo aganizila, nambho Mnungu siwakung’anamuleni maganizo yanu kwa kuganizila bwino. Pamenepo ndipo simkhoze kujhiwa icho wafuna Mnungu ni kujhiwa chindhu chili cha bwino, ilo limkwadilicha ni kuchita ngati umo ifunikila.
Chimwecho simudavomela kusiya kuchita chindhu cha bwino, ndande wandhu wina akamba kuti ni chindhu choipa.
Mchele ni wabwino, nambho ngati ukataiza kukoma kwake, siuthilidwe chiyani kuti ukomenjho? Mkhale ngati mchele uwo ukoma, ni mkhale kwa mtendele ni achanjanu."