Publicidade

Efésios 4

Umojhi wa wandhu okhulupilila

1 Ndiipo ine nili omangidwa ndande ya kwatumikila Ambuye, nikupembhani kupunda mukhale ngati umo Mnungu wakutanilani. 2 Mkhale ojhichicha ni apole, mlimbilane mitima mwachinawene kwa mwachinawene kwa chikondi. 3 Limbichani umojhi wa Mzimu wa Mnungu, ni mkhale kwa mtendele pakati panu. 4 Kuli ni thupi limojhi ni mzimu umojhi, ngati umo kukhulupilila kuli kumojhi uko mwatanidwila ni Mnungu uyo wali mmojhi. 5 Kuli ni Ambuye amojhi, kukhulupilila ni kumojhi ni ubatizi niumojhi, 6 kuli ni Mnungu mmojhi, Atate waonjhe yao alamulila vonjhe, wachita njhito kwa wonjhe ni wali kwa wonjhe.

7 Kila mmojhi wathu walandila mwawi wa Mzimu wa Mnungu kuchokana ni umo Kilisito wampachila. 8 Ndendande yalembedwa mumalembo ya Mnungu,

"Yapo adakwela kumwamba kupunda,

adaatenga omangidwa,

wadapacha wandhu mbhaso."

9 Ndiipo yapo ikambidwa, "Wadakwela kumwamba," mate yake chiyani? Mate yake ni kuti, poyamba wadachika mbaka panjhi pajhiko. 10 Chipano mmeneyo uyo wachika nde uyo wadakwela kumwamba kupunda, dala waenele kila pamalo. 11 Nde uyo wapacha wandhu mbhaso za Mzimu wa Mnungu, wina kukhala atumwi, wina alosi wina olalikila Uthenga Wabwino, wina abusa ni wina oyaluza. 12 Adachita chimwecho ndande ya kwakonjekela wandhu wonjhe a Mnungu, kwa njhito ya kumtumikila Kilisito chimwecho okhulupilila onjhe akhala nganganga ngati umo lili thupi la Kilisito. 13 Chimwecho ife tilunjane ni kukhala chindhu chimojhi kwa chikhulupi ni kumjhiwa Mwana wa Mnungu, tikhale wandhu okwanila ni tikhoze kufikila kukwanila kwa Kilisito mwene wake. 14 Chimwecho sitikhalanjho ngati wana akhanda, nitipelekedwa uku ni uku ni mayaluzo ya kila mtundu, ya oyaluza aunami yao alakwicha wina. 15 Nambho ngati tikauchota uzene kwa mtima wa chikondi sitikule chizimu ni sitimfikile Kilisito pa vindhu vonjhe, iye nde mlamuli wathu. 16 Kwa kuchogozedwa ni Kilisito, thupi lonjhe likalunjidwa ni kugwilizidwa pamojhi, kwa mthandizo wa kila chiwalo. Chipano, kila chiwalo chichita njhito yake, thupi lonjhe likula lene ni kujhikonja muchikondi.

Umoyo wachipano ni umowo wakale

17 Chimwecho, nikuonyani kwa ulamulilo uwo napachidwa ni Ambuye. Msadakhalanjho ngati wandhu yao samjhiwa Mnungu, maganizo yao yali yoipa. 18 Njelu zao zili mumdima, alipatali ni umoyo wa Mnungu ndande ya usabobwa wao ni mitima yao yolimba. 19 Apanduka, alibe njhoni, ali ni ukhalo woyipa, ni apapalikila kupunda vindhu va manyazi va kila mtundu. 20 Nambho anyiimwe simudajhiyaluze chimwecho kwa nghani ya Kilisito. 21 Anyiimwe mwazivela bwino nghani zake, muli ochatila wake mdayaluzidwa mayaluzo ya uzene ya nghani za Yesu. 22 Mudayaluzidwa muvisiye vichito vanu voipa ivo madavichita kale, ngati mujha mundhu wavulila njalu ni kuisiya, vichito ivo vimawanangidwa ni khumbilo launami. 23 Mmizimu mwanu ni mmaganizo yanu mving'anamule vikhale va chipano. 24 Mkhale ni umoyo wa chipano, ngati umo mmungu wadakuumbani, mlingane niiye uku muli ovomelezeka kupunda ni kukhala umo ifunukila.

25 Chimwecho, usiyeni unami. Kila mmojhi wafunika wamkambile mnjake uzene, ndande kila mmojhi ni chiwalo cha Kilisito. 26 Mkakwiya, mbhwai yanu siidakuchitichani mchite machimo, ni simdalongeza ni mbhwai siku la mbhumbhu mbaka yapo jhuwa yapo libila, 27 dala simudampacha Satana malo. 28 Uyo wakuba, siwadabanjho, nambho wayambe kuchita njhito yabwino kwa manja yake, dala wakhale ni chindhu cha kumthangatila osauka. 29 Simudakamba mawu yoipa, nambho mawu yanu yajhikhala ya kwathangatila wina kuchokana ni icho afuna, dala yathangatile yawo akuvelani. 30 Simudamdandaulicha Mzimu wa Mnungu, pakuti Mzimu umeneo ni chizindikilo cha Mnungu kwanu kuti anyiimwe ni wandhu wake, ni uchimikizo ndande ya siku la uomboli. 31 Chimwecho siyani kukhala ni dungulila, ipilo, mbhwai, pokoso ni matukwano ni msiye kila mtundu wa voipa. 32 Mkhale ni mtima wa bwino ni kulengelana lisungu, kila mmojhi wamlekelele mnjake ngati Mnungu umo wakulekelelani anyiimwe kwa kupitila ya Kilisito.

Veja também

Publicidade
Efésios
Ver todos os capítulos de Efésios
Bíblia Online Bíblia Online

Bíblia Online • Versão: 2026-06-16_18-40-07-