Evangelização
A evangelização é a missão suprema da Igreja. Jesus mandou: ide por todo o mundo e pregai o evangelho a toda criatura. O evangelho é poder de Deus para a salvação de todo aquele que crê.
A Grande Comissão
Ide, fazei discípulos de todas as nações. Jesus confiou a seus seguidores a missão de levar a boa notícia ao mundo inteiro.
Chipano pitani kwa wandhu maiko yonjhe, mkaachite kukhala oyaluzidwa, mkaabatize kwa jhina la Atate ni la Mwana ni la Mzimu Woyela, ni mwaayaluze kuyagwila yonjhe yayo nakulamulilani. Zenedi, ine nili pamojhi namwe muyaya mbaka mathelo ya jhiko la panjhi."
Chimwecho wadaakambila, "Pitani kujhiko lonjhe la panjhi, mkalalikile wandhu wonjhe Uthenga Wabwino.
Nambho simujhazidwe mbhavu yapo siwajhe kwanu Mzimu woyela, ni anyiimwe simukhale amboni wanga mmijhi ya Yelusalemu, Yudea yonjhe ni Samaliya, ni jhiko lonjhe lapanjhi."
"Anyiimwe ni dangalila la jhiko! Ni ngati nyumba iyo yamangidwa pamwamba pa phili siukhoza kubisika.
Mchele wa chinyope ni dangalila
"Anyiimwe ni mchele wa chinyope wa jhiko. Nambho mchele wa chinyopeo ngati wasukuluka sikomelechedwe ni chiyani? Ulibe njhito. Siutaidwe kubwalo nikupondedwa ni wandhu."
Wandhu saakweleza nyali ni kuikupika kwa debe. Nambho iyikidwa pamwamba poikila nyali kuti imulikile wandhu wonjhe yao ali mnyumba. Chimwecho dangalila lanu liwale pamaso pa wandhu kuti apenye vichito vanu vabwino ni kwaakweza Atate wanu akumwamba."
Kuchokela nyengo imeneyo Yesu wadayamba kulalikila niwakamba, "Siyani kuchita machimo pakuti ufumu wa kumwamba wawandikila!"
O poder do evangelho
O evangelho é poder de Deus para a salvação. A fé vem pelo ouvir, e o ouvir pela Palavra de Cristo.
Mbhavu ya uthenga wa bwino
Ine siniona njhoni kuuzila uthenga wa Bwino, wene ni mbhavu ya Mnungu, iyo yaombola wandhu wonjhe amkhulupilila Yesu. Kuyambila Ayahudi ni anyiawo osati ayahudi.
Chimwecho, chikhulupi chichokana ni kuvela Uthenga Wabwino, ni uthenga umeneo uchokana ni mawu la Kilisito.
Pajha nidali namwe, nidachita maganizo yanga yaiwalile kila kandhu ila Yesu Kilisito yokha ni nyifa yake pa mtanda.
Kuhyuka kwa Yesu
Chipano nifuna kukumbuchani anyiimwe abale wanga, ujha Uthenga Wabwino nidakulalikilani, namwenjho mudaikhulupilila, ni kuima nganganga. Kupitila Uthenga Wabwino mulamichidwa, ikakhala ngati mupotela njhito Uthenga uwo nidakulalikilani, ila ngati simusiye, kukhulupilila kwanu kudali kwachajhe.
Testemunhar e proclamar
Estai sempre preparados para responder com mansidão a todo aquele que pedir razão da vossa esperança.
Mkakondana, wandhu onjhe sajhiwe kuti anyiimwe nde oyaluzidwa wanga."
Atate wanga apachidwa ulemelelo yapo mchita vindhu ivo vakwadilicha Amnungu, namwe simukhale oyaluzidwa wanga.
Ili nde lamulo ilo atipacha Ambuye,
‘Nakuchitani kukhala dangalila kwa wandhu osati Ayahudi,
kuti wandhu onjhe ajhiko la panjhi aomboledwe.’"
Nambho ata ngati wandhu sianiphe ine, palibe phindu kwa ine. Nambho icho nichifuna ni kukwanilichape njhito iyo anituma Ambuye Yesu
"Mzimu wa Ambuye uli mkati mwanga,
pakuti wanisangha
kwaakambila wosauka uthenga wabwino.
Anituma kuti nauzile wandhu womangidwa ufulu wao,
ni wosapenya akhoze kuonanjho,
ni kwaapacha ufulu yawo aoneledwa.
Yesu wadakamba, "Zenedi nikukambiulani, kila mundhu uyo waisiya wandhu amnyumba yake, kapina mbale wake, kapina mlongo wake, kapina maye wake, kapina atate wake, kapina wana wake kapina minda yake ndande yaine ni ndande ya Uthenga Wabwino, siwalandile vindhu vochuluka pa ndhawi ya saino. Siwalandile nyumba, abale, alongo, maye, wana ni minda ni mavuto, ni masiku yayo yakujha siwalandile umoyo wa muyaya.
Pakuti mundhu uyo wafuna kuuombola umoyo wake, siwautaize, nambho mundhu uyo siwautaize umoyo wake ndande yanga ni kwa ndande ya Uthenga Wabwino, siwauombole.
Fazer conhecer
Dai graças ao Senhor, invocai o seu nome, fazei conhecidas as suas obras entre os povos.