Marido e mulher
O casamento é aliança sagrada entre marido e mulher, instituída por Deus desde o Éden. A Bíblia define papéis complementares fundados em amor, respeito e fidelidade mútua.
Instituição divina
Deus criou homem e mulher e os uniu em uma só carne. O casamento é projeto divino que reflete o amor de Cristo pela Igreja.
Yesu wadaayangha, wadakamba, "Bwanji, simudasome Mmalembo Yoyela kuti poyamba Mnungu wadamuumba mundhu wammuna ni wamkazi? Mnungu wadakamba, ‘Pandande iyi mundhu wammuna siwaasiye atate wake ni maye wake ni kulunjana ni mkazake, ni awili yawa siakhale thupi limojhi.’ Chimwecho, anyiiwo osati awilinjho, nambho thupi limojhi. Icho wachilunjanicha Mnungu, mundhu siwadachisiyanicha."
Papéis no casamento
O marido ama e a mulher respeita. Ambos se submetem voluntariamente a Deus e um ao outro, em parceria e unidade.
Anyiimwe wachimuna, mjhakonda achakazanu ngati Kilisito umo wadalikondela gulu lake, wadajhichocha njhembe ndande yawo, dala kwa mawu lake, walipatule kwa Mnungu kwa kulichuka mumajhi, dala wapate gulu la wandhu amkhulupilila, ilo la sanghidwa ndande ya Mnungu ni labwino, gulu ilo lilibe machimo, kupunduka kapina chilichonjhe cha mtundu umeneo. Chimwecho wachimuna afunika kwakonda achakazao ngati matupi yawo. Uyo wamkonda mkazake mmeneyo wajhikonda mwene. Palibe mundhu uyo waliipila thupi lake, nambho walidyecha ni kuliveka. Nde umo Kilisito walisungila gulu lake,
Anyiimwe wachikazi mjhavela achamunanu ngati kwa vela Ambuye Yesu. Mate yake wammuna nayo wali ni ulamuli kwa mkazake, ngati umo Kilisito wali ni ulamuli kwa gulu la wandhu amkulupilila Kilisito, ndande Kilisito mwene wake nde waliombola gulu limenelo ni nde thupi lake. Ngati umo gulu la wandhu amkhulupilila Kilisito limvelela iye, chimchijha wachikazi ajhavela achamunao kwa vindhu vonjhe.
Nambho kila wammuna ifunika wamkonde mkazake ngati mwene wake ni wamkazi wafunika kumsamala mmunake.
Fidelidade e união
O casamento é honroso e deve ser preservado com fidelidade. O cordão de três dobras não se rompe facilmente.
Permanecer juntos
O que Deus uniu, o homem não separe. A Bíblia protege o casamento e orienta sobre convivência, perdão e perseverança conjugal.
Mayaluzo ya nghani ya Ukwati
Chipano, kuchokana ni zijha nghani mdalemba.
Anyiimwe mdafunjha kuti ni mbasa wammuna siwadakwata. Nambho chimo la chigololo ni loyipa, chimwecho kila wammuna wakhale ni wamkazi wake, ni kila wamkazi wakhale ni wammuna wake. Wammuna wachite umo ifunikila kwa mkazake, ni wamkazi wachite umo ifunikila kwa mmunake, ni kila mmojhi wamkwaniliche mnjake icho chifunika. Wamkazi walibe lamulo pamwamba pa thupi lake, nambho mmunake wali nilamulo pamwamba pa thupi la mkazake, chinchijha wammuna nayonjho walibe lamulo pamwamba pathupi lake, nambho mkazake wali nilamulo pa mwamba pathupi la mmunake. Msadamanana nambho ikakhala mwavomelezana dala mpheze ndhawi ya mapembhelo, ndiipo mbwelelenjho ili Mdani wa Mnungu siwadapheza kukuikani mmayeso ndande ya kulepela kuchekeleza mafuno yanu.
Nambho kwa anyiwajha akwata nili ni lamulo. Wamkazi siwadasiyana ni mmunake, nambho ikakhala wamkazi wasiyana nimmunake, siwada kwatiwa, kapina wabwelelane ni mmunake, ni wammuna siwadalemba kalata ya kumsiya mkazake.
Nambho, wammuna kapina wamkazi siwadakhulupile wafuna kumsiya mnjake uyo wakhulupilila, chimwecho wachite chimwecho. Pakuchita chimwecho, wamkazi kapina wammuna wakhulupila siwamangika ndande Mnungu watitana tikhale ni umoyo wa mtendele. Iwe wamkazi wamkhulupilila Yesu ujhiwa bwanji, ngati siumuombola mmunako? Kapina iwe wammuna ujhiwa bwanji ngati siumuombola mkazako?
Kwa chifani, wamkazi uyo wakwatiwa wamangidwa ni thauko ndhawi yonjhe yapo mmunake wakhala wamoyo, nambho mmunake wakamwalila, thauko limenelo silimmanganjho wamkazi mmeneyo.