Sexo
A Bíblia trata a sexualidade como um presente de Deus para o contexto do casamento. As Escrituras celebram a intimidade conjugal e orientam sobre pureza e santidade sexual.
A sexualidade no plano de Deus
Desde a criação, Deus projetou a intimidade sexual como expressão de amor entre marido e mulher, abençoando a união conjugal.
Yesu wadaayangha, wadakamba, "Bwanji, simudasome Mmalembo Yoyela kuti poyamba Mnungu wadamuumba mundhu wammuna ni wamkazi? Mnungu wadakamba, ‘Pandande iyi mundhu wammuna siwaasiye atate wake ni maye wake ni kulunjana ni mkazake, ni awili yawa siakhale thupi limojhi.’ Chimwecho, anyiiwo osati awilinjho, nambho thupi limojhi. Icho wachilunjanicha Mnungu, mundhu siwadachisiyanicha."
A santidade na intimidade
O leito conjugal é honroso. A Bíblia celebra a alegria da intimidade dentro do casamento e orienta o casal ao amor e respeito mútuo.
Wammuna wachite umo ifunikila kwa mkazake, ni wamkazi wachite umo ifunikila kwa mmunake, ni kila mmojhi wamkwaniliche mnjake icho chifunika. Wamkazi walibe lamulo pamwamba pa thupi lake, nambho mmunake wali nilamulo pamwamba pa thupi la mkazake, chinchijha wammuna nayonjho walibe lamulo pamwamba pathupi lake, nambho mkazake wali nilamulo pa mwamba pathupi la mmunake.
Nambho ngati simukhoza kuchekeleza makhumbilo yanu, chimwecho mkwate kapina kukwatiwa, pakuti mbasa kukwata kapina kukwatiwa kusiyana nikuhla ni kukhumbila.
Mujhiwa kuti mathupi yanu ni viwalo va thupi la Kilisito. Mukhoza kutenga chiwalo cha thupi la Kilisito ni kuchichita malo ya thupi la hule? Siikhozeka! Pakuti uyo walunjana ni hule wakhala thupi limojhi ni huleyo yalembedwa mmalembo ya Mnungu, "Nao awili akhala thupi limojhi." Nambho iye walunjana ni Ambuye wakhala mzimu umojhi ni Ambuye.
Pureza sexual
Deus nos chama à santificação e à fuga da imoralidade. O corpo do cristão é templo do Espírito Santo e deve ser tratado com honra.
Chithaweni chigololo. Machimo yina yonjhe wachita mundhu wachita kubwalo kwa thupi lake, nambho mundhu uyo wachita chigololo wachita mkhati mwathupi lake mwene wake. Simujhiwa kuti mathupi yanu ni nyumba ya Mzimu Wamnungu, uwo ukhala mkati mwanu ni uwo mwapachidwa ni Mnungu? Mathupi yanu osati yanu mwachinawene nambho ni ya Mnungu, pakuti mdaghulidwa kwa mtengo wa ukulu. Tumilani matupi yanu kwa ulemelelo wa Mnungu.
Anyiimwe ni wandhu a Mnungu, chimwecho chighololo, ukhalo waliyojhe woipa kapina chipili, sividakhala pakati panu, pakuti anyiimwe ni wandhu a Mnungu.
Nambho ine nikukambilani kuti uyo siwampenye wamkazi kwa kumkhumbila wathochita chigololo mumtima mwake.
Sitidakhala wandhu ochita mapwando ya kumwa mowa ni kulojhela, ukazuzu, chigololo, ndewo ni njhanjhe.
Achitadama kuti ali ni ekima, nambho ni asabwabwa. Asiya kumlambila Mnungu wa muyaya, ni pambuyo pake, avilambila viboliboli vili chifani cha mundhu uyo wamwalila, chifani cha zinyama, mbalami ni vokwawa.
Ndande imeneyo, Mnungu wasiya achate khumbilo loipa la mitima yao, ni kuchitilana vindhu va njhoni achinawene kwa achinawene. Aung’anamula uzene wa Mnungu ni kuuchita ukhale unami, achilemekeza ni kuchilambila choumbidwa ni Mnungu pambuyo pa kumlambila Mnungu mwene, uyo idafukika kulambilildwa muyaya! Ikhale chimwecho.
Chipano, Mnungu waasiya achate khumbilo loipa. Wachikazi ang’anamula matupi yawo, ni kutumila mosafunikile kwa kukhumbilana achinawene kwa achina wene. Ni wachimuna chimwecho, asiya kukhumbilana wamnuna ni wamkazi, akhumbilana anyiiwo kwa anyiiwo. Wachimuna achitilana vindhu va njhoni, chimwecho saalangidwe kuchokana ni vichito vao voipa.