Pular para o conteúdo
Publicidade

Resultados da busca por "esperança"

7 resultados encontrados

  1. Romanos 8

    Nyanja
    Capítulo 8
    Mostrando versículos 24–35 de 39

    24Pakuti kwa kukhulupila kumeko ife taomboledwa. Nambho kukhulupilila kulibe mate ngati tichiona chijha tichikhulupilila. Pakuti yani wakhulupilila chijha wachiona?

    25Ngati tichikhulupila icho tilibe, chimwecho sitichilindile kwa kuchilimbila mtima.

    35Niyani wakhoza kutiika patali nichikondi cha Kilisito? Bwanji ni kulaga, kapina mavuto, kapina njala, kapina kutedwa njhalu, kapina kuofyedwa kuphedwa?

  2. Atos 3

    Nyanja
    Capítulo 3
    Mostrando versículos 5–23 de 26

    5Mundhu yujha wadaapenya niwalindilila kupata kandhu kuchokela kwa anyiiwo.

    16Kwa kulikhulupilila jhina la Yesu, mundhu uyu mumuona ni kumjhiwa wapachidwa mbhavu. Chikhupililo cha Yesu nde icho chamlamichilatu mundhu uyu, ngati umo mumuonela mwaonjhe."

    23Mundhu waliyonjhe uyo siwamuvela mlosi mmeneyo, siwapatulidwe kuchokela kwa wandhu a Mnungu ni kuphedwa.’

  3. Gálatas 3

    Nyanja
    Capítulo 3
    Mostrando versículos 9–25 de 29

    9Chipano, wajha akhulupilila apachidwa mwawi pamojhi ni Ibulahimu uyo wadakhulupilila.

    23Kukhulupilila yapo kudali sikudajhe, tidamangidwa ni kulondedwa ni thauko, timalindilila kukhulupilila kumeneko kuikidwe padanga.

    25Chipano tikhoza kukhulupilila Kilisito, chimwecho ife sitichogozedwanjho ni Thauko.

  4. Gálatas 5

    Nyanja
    Capítulo 5
    Mostrando versículos 5–9 de 26

    5Pakuti ife tilindilila kwa chikhulupilila ni kwambhavu ya Mzimu, tichitidwe wovomelezeka kwa njila ya kumkhulupilila Kilisito.

    7Mmayendekela bwino! Yani basi, wakuchekelezani simdauvela uzene?

    9Unami pang’ono uwananga mayaluzo yonjhe ya uzene!

  5. Mateus 26

    Nyanja
    Capítulo 26
    Mostrando versículos 37–46 de 75

    37Wadatenga Petulo ni wana awili Azebedayo, wadayamba kuva chizoni ni kulaga mumtima.

    44Chimwecho wadaasiyanjho ni kupita kupembhela kakatatu ni wakamba mau yamweyajha.

    46Imani tijhipita. Yujha waning’anamuka watokujha."

  6. Mateus 21

    Nyanja
    Capítulo 21
    Mostrando versículos 22–46 de 46

    22Mukakulupilila chindhu chilichonjhe simpembhe mmapembhelo, simulandile."

    38Nambho wajha alimi yapo adamuona mwanayujha adakambilana, ‘Uyu nde olanja, majhani timphe dala titenge kulanja kwake’

    46Chimwecho adafuna njila ya kumgwilila nambho adaopa wandhu ndande wandhu adamkhulupilila kuti Yesu wadali mlosi.

  7. Gálatas 6

    Nyanja
    Capítulo 6
    Mostrando versículos 7–16 de 18

    7Simdanyengeka, Amnungu sachitidwa chipongwe. Icho wavyala mundhu nde icho siwakolole

    15Kuchitidwa mdulidwe kapina kosachitidwe mdulidwe asati chindhu chamate, chamate ni kukhala choumbidwa cha chipano.

    16Niwonjhe yawo sakhulupilile, nafunila mtendele ni lisungu ni kwa wandhu a Mnungu Izilaeli.

Léxico (correspondência exata) Semântico (correspondência relacionada) Versículos omitidos Contexto do capítulo