Pular para o conteúdo
Publicidade

Resultados da busca por "esperança"

6 resultados encontrados

  1. Atos 3

    Nyanja
    Capítulo 3
    Mostrando versículos 5–16 de 26

    5Mundhu yujha wadaapenya niwalindilila kupata kandhu kuchokela kwa anyiiwo.

    15Ndiipo mudampha mundhu uyo wadali chiyambo cha umoyo, nambho Mnungu wadamuhyukicha. Ife ni mboni ni tifotokoza ivo vidachokela.

    16Kwa kulikhulupilila jhina la Yesu, mundhu uyu mumuona ni kumjhiwa wapachidwa mbhavu. Chikhupililo cha Yesu nde icho chamlamichilatu mundhu uyu, ngati umo mumuonela mwaonjhe."

  2. Gálatas 3

    Nyanja
    Capítulo 3
    Mostrando versículos 7–23 de 29

    7Chipano mjhiwe kuti wandhu yawo amkhulupilila Mnungu, achamenewo nde wana azene a Ibulahimu.

    9Chipano, wajha akhulupilila apachidwa mwawi pamojhi ni Ibulahimu uyo wadakhulupilila.

    23Kukhulupilila yapo kudali sikudajhe, tidamangidwa ni kulondedwa ni thauko, timalindilila kukhulupilila kumeneko kuikidwe padanga.

  3. Mateus 26

    Nyanja
    Capítulo 26
    Mostrando versículos 28–46 de 75

    28uwu nde mwazi wanga uwo uchimikiza chipangano, umwazika ndande ya ambili dala machimo yao yalekeleledwe.

    44Chimwecho wadaasiyanjho ni kupita kupembhela kakatatu ni wakamba mau yamweyajha.

    46Imani tijhipita. Yujha waning’anamuka watokujha."

  4. Gálatas 6

    Nyanja
    Capítulo 6
    Mostrando versículos 7–16 de 18

    7Simdanyengeka, Amnungu sachitidwa chipongwe. Icho wavyala mundhu nde icho siwakolole

    15Kuchitidwa mdulidwe kapina kosachitidwe mdulidwe asati chindhu chamate, chamate ni kukhala choumbidwa cha chipano.

    16Niwonjhe yawo sakhulupilile, nafunila mtendele ni lisungu ni kwa wandhu a Mnungu Izilaeli.

  5. Romanos 8

    Nyanja
    Capítulo 8
    Mostrando versículos 24–35 de 39

    24Pakuti kwa kukhulupila kumeko ife taomboledwa. Nambho kukhulupilila kulibe mate ngati tichiona chijha tichikhulupilila. Pakuti yani wakhulupilila chijha wachiona?

    25Ngati tichikhulupila icho tilibe, chimwecho sitichilindile kwa kuchilimbila mtima.

    35Niyani wakhoza kutiika patali nichikondi cha Kilisito? Bwanji ni kulaga, kapina mavuto, kapina njala, kapina kutedwa njhalu, kapina kuofyedwa kuphedwa?

  6. 1 Coríntios 12

    Nyanja
    Capítulo 12
    Mostrando versículos 8–19 de 31

    8Mzimu umpacha mundhu mmojhi mawu la ekima, ni mwina mawu lojhiwa umowakondela Mzimu mmeneyo.

    9Mzimu umweo umpacha mwina kukhoza kukhulupilila kwa kukulu, ni mwina wampacha kukhoza kulamicha odwala.

    19Ngati viwalo vonjhe vidakali chiwalo chimojhi thupi lidakali kuti?

Léxico (correspondência exata) Semântico (correspondência relacionada) Versículos omitidos Contexto do capítulo