1 Siku limojhi Petulo ni Yohana amapita ku Nyumba ya Mnungu kupembhela ndhawi ya saa tisa usana. 2 Ndiipo kudali mundhu mmojhi uyo wandendele kuyambila kubadwa kwake. Kila siku wamatengedwa ni kuikidwa pakhomo la Nyumba ya Mnungu ilo limatanidwa, Khomo Labwino, kuti wajhipembha ndalama kwa wandhu yawo amalowa ni kutuluka Mnyumba ya Mnungu. 3 Mundhu mmeneyo yapo wadaaona Petulo ni Yohana naalowa pa nyumba ya Mnungu, wadaapembha ampache ndalama. 4 Petulo ni Yohana adampenyechecha mundhu yujha, ndiipo Petulo wadamkambila, "Tipenye ife." 5 Mundhu yujha wadaapenya niwalindilila kupata kandhu kuchokela kwa anyiiwo. 6 Nambho Petulo wadamkambila, "Nilibe ndalama, nambho nikupacha chindhu icho nilinacho. Mu jhina la Yesu wa ku Nazaleti ima ni ujhiyenda." 7 Ndiipo Petulo wadamgwila yujha mundhu kwa jhanja lake lakwene ni kumuimicha, ndhawi imweyo myendo yake ni vifundo va myendo yake vidali ni mbhavu. 8 Wadalumbha ni kuima ni kuyamaba kuyenda. Ndiipo wadalowa pa Nyumba ya Mnungu pamojhi ni Petulo ni Yohana, niwayenda ni kuyamika ni kumtamanda Mnungu. 9 Wandhu yawo adali pajha adamuona iye niwayenda ni kumtamanda Mnungu. 10 Yapo adamjhiwa kuti nde yujha wamakhala pakhomo la Nyumba ya Mnungu ilo litanidwa, Khomo Labwino, ni kupembha ndalama, adazizwa kupunda ni sadajhiwe icho chimayendekela.
11 Mundhu yujha wadalamichidwa yapo wamachogozana ni Petulo ni Yohana. Wandhu wonjhe adadabwa kupunda, adaathamangila mbaka kumalo kumatanidwa pa khumbi la Solomoni. 12 Ndiipo Petulo yapo wadaona kuti wandhu asonghana, wadaakambila, "Anyiimwe wandhu a ku Izilaeli, ndande yanji muvizizwa vindhu ivi? Bwanji mutipenyechecha kwa kutizizwa ngati ife tamchita mundhu uyu wayende kwa mbhavu zathu, kapina ndande ife abwino pachogolo pa Amnungu? 13 Mnungu wa Atate wathu Ibulahimu ni Isaka ni Yakobo, wadamuhyucha Yesu Mbuye wathu. Nambho anyiimwe mudampeleka kwa akulu a maulamulilo ni kumukana pamaso pa Pilato, ingakhale Pilato wadafuna kumsiilila Yesu. 14 Anyiimwe mudamkana Yesu, mundhu yujha Woyela ni wovomelezeka pamaso pa Mnungu, mdampembha Pilato wamasulidwe wakupha yujha. 15 Ndiipo mudampha mundhu uyo wadali chiyambo cha umoyo, nambho Mnungu wadamuhyukicha. Ife ni mboni ni tifotokoza ivo vidachokela. 16 Kwa kulikhulupilila jhina la Yesu, mundhu uyu mumuona ni kumjhiwa wapachidwa mbhavu. Chikhupililo cha Yesu nde icho chamlamichilatu mundhu uyu, ngati umo mumuonela mwaonjhe."
17 "Chipano achabale wanga, nijhiwa kuti anyiimwe mudachita popande kujhiwa ngati umo adachitila achogoleli wanu. 18 Nambho kwa kupitila yaya Mnungu wadakwanilicha chijha wadalosa kupitila alosi wake wonjhe, kuti Kilisito siwapachikidwe. 19 Chimwecho lapani, mumbwelele Mnungu, kuti wakulekeleni machimo yanu. 20 Mkachita chimwecho, simchuluchidwe mbhavu za Mzimu Woyela kuchokela kwa Ambuye, nawo samtume Yesu Kilisito uyo amsangha, 21 uyo wamafunika kulandilidwa kumwamba mbaka ijhe ndhawi yochita kila kandhu chikhale cha chipano. Nghani izi zimakambidwa ni Mnungu kupitila alosi wake woyela kuyambila chiyambo cha jhiko la panjhi. 22 Chimchijha, Musa wadakamba, ‘Ambuye Mnungu wanu siwakupacheni mlosi uyo siwachokele pakati panu. Namwe mufunika kumvechela mmeneyo kwa kila chindhu icho siwakukambileni. 23 Mundhu waliyonjhe uyo siwamuvela mlosi mmeneyo, siwapatulidwe kuchokela kwa wandhu a Mnungu ni kuphedwa.’ 24 Yetu, alosi wonjhe kuyambila Samweli ni wajha adachata, wonjhe adalosela kuhusu nyengo zino. 25 Yajha adayakamba Amnungu kwa njila ya alosi ndande yanu, ni anyiimwe muli muyameneyo adayakamba Amnungu ni azee wanu, ngati umo wamkambila Ibulahimu, ‘Kwanjila ya mbadwa wako wandhu wonjhe apajhiko sapachidwe mwawi.’ 26 Ndiipo Amnungu adamuhyukicha uti mtumuki wake ni kumtuma kwa anyiimwe, kuti wakupacheni mwawi kwa kukuchitani kila mmojhi wanu wasiye vichito vake voipa."