1 Poolo ni Sila adamanga ulendo kwa kupitila mijhi ya Amfipoli ni Apoloniya. Adafika kumujhi wa Tesalonike uko kudali nyumba yokomanilana Ayahudi. 2 Poolo wadalowa mnyumba yokomanilana Ayahudi, ngati umo lidali khalidwe lake. Wadakambilana ni wandhu nghani za Malembo Yoyela kwa Masiku yatatu yo Pumulila wadaakambila, 3 uku ni wafotokozela malembo kwa kualangiza kuti Kilisito wamafunika kufa ni kuhyuka, niwakamba, "Uyu Kilisito nikukambilani nghani zake nde Yesu." 4 Ayahudi akumojhi adaakhulupilia Poolo ni Sila ni adalamula kulunjana nawo. Chiwelengelo chidachuluka cha Agiliki yawo amamlambila Mnungu wazene ni wachikazi ambili yawo amalemekezedwa mjhiko limenelo naonjho adalunjana nawo.
5 Nambho Ayahudi wina adali ni njhanje, adaatenga wandhu woipa apamalo yapo wandhu amasonhgana, adalunjhana nawo ni kuyamba kupeleka chiwawa. Adapanga gulu ni kuyambicha chiwawa mmujhi. Adapita kukhomo kwa Yasoni kwaafunafuna Poolo ni Sila, kuti waapeleke pachogolo pa wandhu. 6 Nambho saadakomane, adamgwila Yasoni pamojhi ni wandhu wina yawo adamkhulupila Kilisito ni kumkwekweta mbaka kwa azee a mujhi ujha uku niapokosela, niakamba, "Wandhu anyiyawa ayambicha chiwawa kila kumalo pajhiko lonjhe, ni chipano afikanjho pamujhi pathu pano, 7 ni Yasoni watokwaasunga mnyumba mwake. Anyiiwo onjhe achuchana ni lamulo la mfumu wa ku Loma, uku niakamba kuti kuli mfumu mwina, uyo watanidwa Yesu." 8 Achogoleli amujhi ni gulu la wandhu Yapo adavela chimwechi, adakwiya kupunda. 9 Wadaakakamiza Yasoni ni wandhu wina yawo adamkhulupilila Yesu achoche ndalama, ndiipo adaasiya apite.
10 Usiku yapo udafika, wajha adamkhulupilila Yesu adaakambila Poolo ni Sila ajhipita ku mujhi wa Beloya. Yapo adaifika kumeneko, adalowa mu nyumba yokomanilana Ayahudi. 11 Ayahudi anyiyawa a ku Beloya amavechecha kupunda kupitilila wajha aku Sesalonike. Adakondwa kupunda yapo adauvela uthenga uwo adakambidwa ni Poolo, ni kila siku amatosoma Malembo ya Mnungu, kuona nagati icho wamakamba Poolo ni chazene. 12 Nambho Ayahudi ambili pamojhi ni wachikazi ni waachimuna a Chigiliki yawo adali achogoleli, adamkhulupilila Yesu. 13 Nambho Ayahudi aku Sesalonike yapo adajhiwa kuti Poolo wamatolalikila Uthenga wa Mnungu mu mujhi wa Beloya, chimchijha adalamula kupita kumeneko. Yapo adafika adachita chiwawa ni kusongezela magulu ya wandhu. 14 Pampajha wajha adamkhulupilila Yesu adampelekeza Poolo mbhepete mwanyanja, nambho Sila ni Timoseo adakhalila ku Beloya. 15 Wajha adampelekeza Poolo, adampelekeza mbaka kumujhi wa Asene. Ndiipo adamsiya, adabwela ku mujhi wa Beloya ni uthenga kuchokela kwa Poolo, Sila ni Timoseo kuti amchate chisanga.
16 Poolo yapo wamaalindilila Sila ni Timoseo mumujhi wa Asene, wadakwiya kupunda ndande wadaona mujhi ujha wachuluka viboliboli va minungu. 17 Chimwecho wadafujhana ni Ayahudi ni wina yawo adali osati Ayahudi mu manyumba yao yokomanilana. Chimchijha siku zonjhe wamakamba ni wandhu yawo amakoma pa danga yayo amakomanilana wandhu ambili. 18 Ndiipo wina yawo amachata ukhalo wa Epukolio ni Asitoiko yawo adali asomi waakulu kupunda adachuchana ni Poolo. Wina adakamba, "Bwanji mundhu uyu wakamba icho siwachijhiwa?"
Wina adakamba, "Iyeyu waoneka ngati wakamba nghani za minungu yachilendo." Adakamba chimwechi ndande Poolo wamalalikila nghani za Yesu ni kuhyuka kwake. 19 Ndiipo adamtenga Poolo ni kupitananayo khumbi ilo limatanidwa Aleopago, niakamba, "Chonde tifokotezelele ganizo ili la chipano ilo uliyaluza. 20 Ivo uvikamba kwatu ni vachilendo, tifuna tijhiwe mate ya vindhu vimenevo." 21 Wandhu aku Asene ni alendo yawo amakhala mmenemo, amatumia ndhawi yao yonjhe kukambilana ni kuvechela maganizo yajha yachipano.
22 Poolo wadaima pachogolo pa khumbi limenelo la Aleopago niwakamba, "Anyiimwe wandhu aku Asene! Icho nichiona pano ilangiza kuti anyiimwe ni wandhu muilambila kupunda minungu yanu. 23 Yapo nimapita mmujhi wanu uku ni uko nidapenya viboliboli va minungu yanu, nikulambila kwanu, nidaona ghuwa limojhi ilo lalembedwa, ‘Kwa mnungu uyo siwajhiwika.’ Ilangiza kuti Mnungu Uyo mumlambila simumjhiwa. Chipano nifuna nikukambileni nghani za Mnungu wa uzene uyo ifunika mumlambile. 24 Nde Mnungu uyo wadaumba jhiko ni vindhu vonjhe vili mkati mwake, ni Ambuye a kumwamba ni jhiko lapanjhi ni siwakhala mnyumba yamangidwa ni wandhu. 25 Iye ndeuyo waapacha wandhu umoyo, mpuyo ni kila chindhu icho achifuna. Siwafuna chithandizo chilichonjhe kuchokela kwa wandhu, iye wali ni kila kandhu icho wandhu achifuna. 26 Mnungu wadayamba kumuumba mundhu mmojhi, ni kupitila kwaiye wadaumba mafuko yonjhe yosiyanasiyana, ni kwaachita akhale malo yonjhe pajhiko. Wadalamula kuchokela poyamba, ndhawi iti ni kuti sakhale wandhu ameneo. 27 Mnungu wadachita chimwechi kuti wandhu amfunefune iye ata ngati kwa kupambasa ni ayese kumpata, pakuti siwakhala kutali ni kila mmojhi wathu, 28 ngati umo wadakambila mundhu mwina,
‘Mkati mwake ife tikhala, tijhikoza ni tilipo.’
Ngati wandhu wina umo adakambila,
‘Ife nafenjho ni wana wake.’
29 Uzene ni kuti ife taonjhe ni wana a Mnungu ni tachokela kwa Mnungu. Chimwecho, tisadaganiza kuti Mnungu walingana ni viboliboli va myala ya mtengo wa ukulu, kapina ndalama kapina vamwala uwo wakonjedwa kwa kusoma ni njelu za mundhu. 30 Mnungu wadachita ngati siwapenya ndhawi zijha wandhu samamjhiwe Mnungu wa zene. Nambho chipano walamula wandhu wonjhe akila kumalo alape ni kumng'anamukila iye, 31 pakuti waika siku ilo siwalilamule jhiko lonjhe kwa haki kupitila mundhu uyo wadamsanghula. Iye walangiza wandhu padanga chindhu chimenecho kwa wandhu pakumuhyukicha Kilisito!"
32 Yapo adavela Poolo niwakamba nghani za kuhyuka, wina wao adayamba kumseka. Nambho wina wao adakamba, "Tifuna kuivelanjho ghani imeneyo." 33 Chimwecho Poolo wadaasiya ni kuchoka. 34 Nambho wandhu wina adachatana ni Poolo ni kumkhulupilila Kilisito. Pakati pawo padali Dionisio mundhu wa khumbi la Leopago ni wamkazi mmojhi uyo wadatanidwa Damali ni wandhu wina.