Pular para o conteúdo
Publicidade

Resultados da busca por "amor"

24 resultados encontrados

  1. Salmos 119

    Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
    Capítulo 119
    Mostrando versículos 64–140 de 176

    64Dziko lapansi ladzaza ndi chikondi chanu chosasinthika,phunzitseni malamulo anu.Teti

    88Sungani moyo wanga molingana ndi chikondi chanu chosasinthika,ndipo ndidzamvera umboni wa pakamwa panu.Lamedi

    140Mawu anu ndi woyera kwambirinʼchifukwa chake mtumiki wanune ndimawakonda.

  2. Romanos 16

    Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
    Capítulo 16
    Mostrando versículos 8–27 de 27

    8Perekani moni kwa Ampliato, amene ine ndimamukonda mwa Ambuye.

    16Mupatsane moni wina ndi mnzake mwachikondi choona.Mipingo yonse ya Khristu ikupereka moni.

    27kwa Mulungu yekhayo wanzeru kukhale ulemerero kwamuyaya kudzera mwa Yesu Khristu! Ameni.

  3. Cânticos 6

    Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
    Capítulo 6
    Mostrando versículos 1–10 de 13

    1Iwe wokongola kuposa akazi onsewa,kodi wokondedwa wakoyo wapita kuti?Kodi wokondedwa wakoyo wakhotera njira itikuti timufunefune pamodzi ndi iwe?Mkazi

    3Wokondedwa wangayo ndine wake ndipo iyeyo ndi wangawanga;amadyetsa ziweto zake pakati pa maluwa okongola.Mwamuna

    10Ndani uyu akuoneka ngati mʼbandakucha,wokongola ngati mwezi, wowala ngati dzuwa,wochititsa mantha ngati gulu la ankhondo mbendera zili mʼmanja?Mwamuna

  4. Salmos 57

    Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
    Capítulo 57
    Mostrando versículos 3–10 de 11

    3Mulungu amanditumizira kuchokera kumwamba ndi kundipulumutsa,kudzudzula iwo amene akundithamangitsa kwambiri.Mulungu amatumiza chikondi chake ndi kukhulupirika kwake.

    8Dzuka moyo wanga!Dzukani zeze ndi pangwe!Ndidzadzuka mʼbandakucha.

    10Pakuti chikondi chanu nʼchachikulu, kufikira ku mayiko akumwamba;kukhulupirika kwanu kwafika ku mitambo.

Léxico (correspondência exata) Semântico (correspondência relacionada) Versículos omitidos Contexto do capítulo