Pular para o conteúdo
Publicidade

Resultados da busca por "esperança"

27 resultados encontrados

  1. Romanos 5

    Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
    Capítulo 5
    Mostrando versículos 2–5 de 21

    2Iyeyo ndiye amene anatsekulira njira mwachikhulupiriro yolowera mʼchisomo mʼmene takhazikikamo. Ndipo tikukondwerera chiyembekezo cha ulemerero wa Mulungu.

    4Ndipo kupirira kumabweretsa makhalidwe, makhalidwe amabweretsa chiyembekezo.

    5Ndipo chiyembekezo chimenechi sichitikhumudwitsa chifukwa Mulungu mwa Mzimu Woyera, amene Iye anatipatsa, wadzaza mʼmitima mwathu ndi chikondi chake.

  2. Lamentações 3

    Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
    Capítulo 3
    Mostrando versículos 21–29 de 66

    21Komabe ndimakumbukira zimenezi,nʼchifukwa chake ndili ndi chiyembekezo.

    26nʼkwabwino kudikira chipulumutso chaYehova modekha.

    29Abise nkhope yake mʼfumbimwina chiyembekezo nʼkukhalapobe.

  3. Jó 6

    Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
    Capítulo 6
    Mostrando versículos 11–25 de 30

    11"Kodi mphamvu zanga nʼzotani kuti ndizikhalabe ndi chiyembekezo?Nanga zoyembekezera zanga nʼzotani kuti ndipirirebe?

    19Anthu oyenda pa ngamira a ku Tema amafunafuna madzi,anthu amalonda apaulendo a ku Seba amafunafuna mwa chiyembekezo.

    25Ndithu, mawu owona ndi opweteka!Koma mawu anu otsutsa akufuna kuonetsa chiyani?

  4. Colossenses 1

    Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
    Capítulo 1
    Mostrando versículos 5–26 de 29

    5Chikhulupiriro ndi chikondi, gwero lake ndi chiyembekezo chomwe muli nacho chodzalandira zimene anakusungirani kumwamba. Munamva kale za zimenezi kudzera mʼmawu a choonadi, Uthenga Wabwino

    23ngati mupitirirabe kukhala mʼchikhulupiriro chanu, okhazikika ndi olimba, osasunthidwa kuchoka pa chiyembekezo chimene munachigwira mu Uthenga Wabwino. Uwu ndi Uthenga Wabwino umene munawumva, umene wakhala ukulalikidwa kwa olengedwa onse a pansi pa thambo, ndi umenenso, ine Paulo ndinakhala mtumiki wake.

    26chinsinsi chimene chakhala chikubisika kwa nthawi ndi mibado, koma tsopano chawululidwa kwa oyera mtima.

  5. Deuteronômio 5

    Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
    Capítulo 5
    Mostrando versículos 2–19 de 33

    2Yehova Mulungu wathu anachita pangano ndi ife ku Horebu.

    17"Usaphe.

    19"Usabe.

  6. Atos 3

    Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
    Capítulo 3
    Mostrando versículos 5–25 de 26

    5Munthuyo anawayangʼanitsitsa kuyembekezera kuti alandira kanthu kuchokera kwa iwo.

    16Mwachikhulupiriro mʼdzina la Yesu, munthu uyu amene mukumuona ndi kumudziwa analimbikitsidwa. Mʼdzina la Yesu ndi chikhulupiriro chimene chili mwa iye chamuchiritsa kwathunthu, monga nonse mukuona.

    25Inu ndinu ana a aneneri ndiponso ana apangano limene Mulungu anachita ndi makolo anu. Iye anati kwa Abrahamu, ‘Anthu onse a pa dziko lapansi adzadalitsika kudzera mwa zidzukulu zako.’

  7. Jó 17

    Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
    Capítulo 17
    Mostrando versículos 1–15 de 16

    1"Mtima wanga wasweka,masiku anga atha,manda akundidikira.

    7Mʼmaso mwanga mwada ndi chisoni;ndawonda ndi mutu womwe.

    15tsono chiyembekezo changa chili kuti?Ndani angaone populumukira panga?

  8. Provérbios 23

    Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
    Capítulo 23
    Mostrando versículos 16–26 de 35

    16Mtima wanga udzakondwerapamene ndidzakumva ukuyankhula zolungama.

    18Ndithu za mʼtsogolo zilipondipo chiyembekezo chakocho sichidzalephereka.

    26Mwana wanga, undikhulupirirendipo maso ako apenyetsetse njira zanga.

  9. Êxodo 20

    Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
    Capítulo 20
    Mostrando versículos 8–15 de 26

    8"Uzisunga tsiku la Sabata kuti likhale lopatulika.

    13"Usaphe.

    15"Usabe.

  10. 1 Coríntios 13

    Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
    Capítulo 13
    Mostrando versículos 4–13 de 13

    4Chikondi nʼcholeza mtima, chikondi nʼchokoma mtima, chilibe nsanje, sichidzikuza, sichidzitamandira.

    7Chimatchinjiriza nthawi zonse, chimakhulupirika nthawi zonse, chimakhala ndi chiyembekezo nthawi zonse, chimapirira nthawi zonse.

    13Ndipo tsopano zatsala zinthu zitatu: chikhulupiriro, chiyembekezo ndi chikondi. Koma chachikulu pa zonsezi ndi chikondi.

  11. Provérbios 19

    Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
    Capítulo 19
    Mostrando versículos 18–22 de 29

    18Langa mwana wako, chiyembekezo chikanalipo;ngati sutero udzawononga moyo wake.

    21Munthu amakonzekera zambiri mu mtima mwake,koma cholinga cha Yehova ndiye chidzachitike.

    22Chimene munthu amafuna ndi chikondi chosatha;nʼkwabwino kukhala wosauka kusiyana ndi kukhala wabodza.

  12. Romanos 8

    Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
    Capítulo 8
    Mostrando versículos 19–25 de 39

    19Pakuti chilengedwe chikudikira ndi chiyembekezo kuonetsedwa poyera kwa ana a Mulungu.

    24Pakuti ife tinapulumutsidwa mʼchiyembekezo ichi. Koma chiyembekezo chimene chimaoneka si chiyembekezo ayi. Kodi ndani amene amayembekezera chimene ali nacho kale?

    25Koma ngati ife tiyembekeza chimene tikanalibe, ndiye kuti tikuyembekeza modekha mtima.

  13. 1 Crônicas 1

    Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
    Capítulo 1
    Mostrando versículos 11–21 de 54

    11Igupto ndiye kholo laAludi, Aanami, Alehabu, Anafutu,

    16Aaravadi, Azemari ndi Ahamati.

    21Hadoramu, Uzali, Dikila

  14. 2 Coríntios 3

    Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
    Capítulo 3
    Mostrando versículos 4–12 de 18

    4Kulimba mtima kumeneku tili nako pamaso pa Mulungu kudzera mwa Khristu.

    8kodi nanga utumiki wa Mzimu sudzaposa apa?

    12Choncho, popeza tili ndi chiyembekezo chotere, ndife olimba mtima kwambiri.

  15. Efésios 1

    Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
    Capítulo 1
    Mostrando versículos 1–18 de 23

    1Paulo, mtumwi wa Khristu Yesu mwachifuniro cha Mulungu.Kulembera oyera mtima a ku Efeso, okhulupirika mwa Khristu Yesu:

    12nʼcholinga chakuti, ife amene tinali oyamba kukhala ndi chiyembekezo mwa Khristu, tiyamike ulemerero wake.

    18Ndimapempheranso kuti maso a mitima yanu atsekuke ndi cholinga choti mudziwe chiyembekezo chimene Iye anakuyitanirani, chuma cha ulemerero chomwe chili mwa anthu oyera mtima.

  16. Salmos 39

    Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
    Capítulo 39
    Mostrando versículos 5–11 de 13

    5Inu mwachititsa kuti masiku anga akhale ochepa kwambiri,kutalika kwa zaka zanga ndi kopanda phindu pamaso panu;moyo wa munthu aliyense ndi waufupi.Sela

    7"Koma tsopano Ambuye kodi ndifunanso chiyani?Chiyembekezo changa chili mwa Inu.

    11Inu mumadzudzula ndi kulanga anthu chifukwa cha tchimo lawo;mumawononga chuma chawo monga njenjete;munthu aliyense ali ngati mpweya.Sela

  17. Salmos 130

    Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
    Capítulo 130
    Mostrando versículos 1–6 de 8

    1Ndikulirira kwa Inu Yehova ndili mʼdzenje lozama;

    5Ndimayembekezera Yehova, moyo wanga umayembekezera,ndipo ndimakhulupirira mawu ake.

    6Moyo wanga umayembekezera Ambuye,kupambana momwe alonda amayembekezera mmawa,inde, kupambana momwe alonda amayembekezera mmawa,

  18. Hebreus 11

    Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
    Capítulo 11
    Mostrando versículos 1–33 de 40

    1Tsopano chikhulupiriro ndi kusakayika konse pa zinthu zimene tikuziyembekeza, ndi kutsimikiza kuti zinthu zimene sitiziona zilipo ndithu.

    2Ndi chikhulupiriro chimenechi makolo athu akale anayamikidwa.

    33amene ndi chikhulupiriro anagonjetsa mafumu, anakhazikitsa chilungamo ndi kulandira zimene zinalonjezedwa. Anatseka pakamwa pa mikango,

  19. Ezequiel 7

    Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
    Capítulo 7
    Mostrando versículos 5–25 de 27

    5"Zimene ndikunena Ine Ambuye Yehova ndi izi:"Chiwonongeko! Chiwonongeko chimene sichinamvekepo!Taona chikubwera!

    6Chimaliziro chafika!Chimaliziro chafika!Chiwonongeko chakugwera.Taona chafika!

    25Nkhawa ikadzawafikiraadzafunafuna mtendere koma osawupeza.

  20. Ezequiel 1

    Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
    Capítulo 1
    Mostrando versículos 14–28 de 28

    14Zamoyozo zinkathamanga uku ndi uko ngati kungʼanima kwa mphenzi.

    17Mikombero ija poyenda inkatha kupita mbali iliyonse yomwe zamoyozo zinayangʼana popanda kutembenuka.

    28Kuwalako kunali ndi maonekedwe a utawaleza mʼmitambo tsiku limene kwagwa mvula.Umu ndi mmene ulemerero wa Yehova umaonekera. Pamene ndinawuona ndinagwa pansi ndipo ndinamva mawu akundiyankhula.

Léxico (correspondência exata) Semântico (correspondência relacionada) Versículos omitidos Contexto do capítulo