Publicidade

Zacarias 7

9 "Yehova Wamphamvuzonse akuti, Muziweruza molungama; muzichitirana chifundo ndi kumverana chisoni. 10 Musamazunze akazi amasiye kapena ana amasiye, alendo kapena osauka. Musamaganizirane zoyipa mʼmitima mwanu.

Veja também

Publicidade
Bíblia Online Bíblia Online

Bíblia Online • Versão: 2026-06-29_22-07-56-