Amor incondicional
O amor incondicional de Deus não depende de mérito humano. Ele nos amou quando ainda éramos pecadores. Esse amor não tem limites, não cobra preço e não pode ser perdido.
Amor sem condições
Deus prova o seu amor em que Cristo morreu por nós sendo nós ainda pecadores. O amor de Deus é gratuito e irrevogável.
Nambho Mnungu wachimikiza kuti watikonda, pakuti yapo tidali tikali amachimo, kilisito wadafa ndande yathu.
Pakuti sikhozekana mundhu kumwalila ndande ya mundhu wa ubwino, nambho mundhu wakhoza kujhichocha kumwalila ndande ya mundhu wabwino. Nambho Mnungu wachimikiza kuti watikonda, pakuti yapo tidali tikali amachimo, kilisito wadafa ndande yathu.
Wandhu wonjhe achita machimo, palibe uyo wali wabwino ni wonjhe ataiza kulemekezedwa ni Mnungu. Nambho kwa mbhaso ya ubwino wa Mnungu, wandhu wonjhe avomelezedwa kuti ni abwino pachogolo pa Mnungu kwa njila ya Yesu Kilisito uyo wadaombola.
Niyani wakhoza kutiika patali nichikondi cha Kilisito? Bwanji ni kulaga, kapina mavuto, kapina njala, kapina kutedwa njhalu, kapina kuofyedwa kuphedwa?
Mateyake Amnungu adaakonda wandhu a jhiko la panjhi ni kumchocha Mwana wao wa yokha, kuti kila uyo wamkhulupilila siwadatayika, nambho wakhale ni umoyo muyaya.
Ife nafe taonjhe timakhala ngati anyiiwo, timachata makhumbilo yathu ya jhiko ni kuchita ivo vikwadilicha matupi ni njelu zathu. Nafe mmayambo tidali ngati anyiiwo, timafunika tilangidwe ni Amnungu.
Nambho Mnungu ni alisungu kupunda. Adatikonda kwa chikondi chachikulu, ata ngati tidamwalila ndande ya machimo, adatichita amoyo pamojhi ni Kilisito. Kwa ubwino wa Mnungu anyiimwe mwaomboledwa.
Amor eterno
Com amor eterno te amei. O amor de Deus é mais largo, mais alto e mais profundo do que podemos compreender.
Amar como Deus ama
O amor é paciente e bondoso. Amai os vossos inimigos. O amor incondicional se expressa no perdão e na compaixão.
Uyo wali ni chikondi waembekeza, wathangatila, uyo wali nichikondi walibe njhanje, walibe dama, kapina kujhiona, uyo wali ni chikondi siwachepa ulemu, uyo wali ni chikondi siwafuna vindhu va kumthangatila mwene, kapina mbhwai za msanga, siwasunga chikumbukilo cha voipa,
mundhu wa chikondi siwakondwela voipa, nambho chikondwela uzene. Mundhu wachikondi wapilila yonjhe, mundhu wa chikondi wakhulupila wina, mundhu wa chikondi waembekeza, ni siwalepela.
Kwakonda adani
"Mwavela kuti idakambidwa kuti, ‘Mkonde mnjako ni umuipile mdani wako.’ Nambho ine nikukambilani akondeni adani wanu ni kwapembhela anyiyao akuvutichani anyiimwe, kuti mkhale wana wa Atate wanu ali kumwamba. Pakuti iye wawalichila jhuwa lake wandhu woipa ni wandhu abwino ni kwanyechela vula wandhu yawo achita ivo vivomelezeka kwa Mnungu ni wandhu yawo saachita vovomelezeka. Bwanji, simupate chikho chanji ngati simwaakonde wajha akukondanipe? Palibe! Pakuti olandila malipilo nawo achita chimwecho. Chinchijha ngati mkaalonjela abale wanupe bwanji, mchita chindhu chanji chachikulu kupitilila wandhu wina? Ata wandhu yawo samjhiwa Mnungu saachita chimwecho. Chimwecho khalani wokwanila ngati Tate wanu wa kumwamba umo wali okwanila."
Akondeni adani wanu
"Nambho nikukambilani anyiimwe munivela, akondeni adani wanu, ni kwachitila yabwino yawo akuipilani. Mwapache mwawi yawo akulosani, apembheleni kwa Mnungu yawo akuchitani voipa.