A carne
A carne representa a natureza pecaminosa que milita contra o Espírito. A Bíblia ensina que os que pertencem a Cristo crucificaram a carne com suas paixões e desejos.
Carne versus Espírito
Os que são segundo a carne inclinam-se para as coisas da carne. O nascido da carne é carne; o nascido do Espírito é Espírito.
Pakuti anyiwajha akhala kwa kulichata thupi, achogozedwa ni maganizo ya thupi, nambho anyiwajha akala ngati ufunila mzimu wa Mnungu, achogozedwa ni maganizo ya mzimu. Maganizo yayo yachogozedwa ni thupi yapeleka nyifa, nambho maganizo yayo yachogozedwa ni Mzimu yapeleka umoyo ni mtendele. Mundhu uyo wachogozedwa ni maganizo ya thupi ni mdani wa Mnungu, siwachata thauko la Mnungu ni siwakhoza kulivela. Wandhu yao achata umo lifunila thupi, sakhoza kumkwadilicha Mnungu.
Nambho anyiimwe simchogozedwa ni thupi, ila mchogozedwa ni Mzimu, ikhalape ngati Mzimu wa Mnungu ukhala mkati mwanu. Chimwecho waliyonjhe uyo walibe Mzimu wa kilisito mmeneyo osati wake Kilisito.
Kukhala kwa mbhavu za Mzimu wa Mnungu
Chipano palibe lamulo la chilango kwa anyiwajha yao muukhalo wao alunjana ni Kilisito. Pakuti thauko la Mzimu ilo lipeleka umoyo kwa kulanjana ni kilisito Yesu, yanilekelela kuchokela mthauko la machimo ilo lipeleka nyifa. Mnungu wadachita chindhu chijha thauko silidakhoze kuchita, ndande ya kuchepekela kwa Mundhu. Mnungu wadamtuma Mwana wake uku wali ni thupi ngati umo tili ife, dala wayachoche machimo kwa thupi lake, ni kwa thupi limwelo wayachoche machimo. Mnungu wadachita chimwecho kuti tikhoze kuchita yajha yafunika ni thauko, kwa kumkhulupilila mzimu wa Mnungu pambuyo pa kuyavela makhumbilo ya matupi yathu.
Pakuti mkakhala ngati umo lifunila thupi, zenedi simmwalile. Nambho ngati mkakhala mkati Mzimu muyaipha machitidwe yanu ya chithupi kwa chizimu simkhale moyo. Wonjhe achogozedwa ni Mzimu wa Mnungu ni wana wa Amnungu.
Chipano najhiwa chimwechi, kuti nifuna kuchita chindhu chabwino, nambho nijhipeza kuti chijha chilichoipa nde ichonisangha. Mumtima wanga, nilikondwela thauko la Mnungu. Nambho niona kuti mkati mwanga kuli thauko lina ilo lichita njhito ilo lichuchana ni maganizo yanga ya bwino. Thauko limenelo linichita kukhala kapolo wa thauko la machimo yayo yachita njhito mthupi mwanga.
Pakuti yapo timakhala ngati wandhupe umo akhalila, makumbilo yayo yadasongezeledwa ni machimo yamachita njhito mmatupi yathu, ni kupeleka nyifa.
Mundhu wabadwa chithupi kwa atate wake ni amake, nambho wabadwa Chizimu kwa Mzimu woyela.
Mzimu wa Amnungu nde uwo uchocha umoyo, thupi silikhoza kandhu. Mawu yayo nakukambilani ni mzimu ni umoyo.
Vencer a carne
Andai no Espírito e não cumprireis os desejos da carne. Os que são de Cristo crucificaram a carne com suas paixões.
Kuchogozedwa ni Mzimu wa Mnungu
Chipano nikamba chimwechi, ukhalo wanu uchogozedwe ni Mzimu wa Mnungu, mkachita chimwecho simuchatanjho makumbilo yoipa.
Vichito va jhiko vijhiwika navo nde ivi, uhule, chigololo, ni ukhalo woyipa, kulambila viboliboli, ufiti, udani, ndewo, njhanje, mbwayi, chipili, mkangano ni kosavana, kosakondwela mwina wakakhala ni chindhu, kulojhela mowa kudya kupunda ni vindhu vili ngati vimenevo. Nikuonyani ngati umo nidakuonyelani mmayambo, wandhu achita yameneyo saupata ufumu wa Amnungu.
Anyiwajha ali ni Kilisito aupachika pamtanda ukhalo wao wa chijhiko pamojhi ni maganizo yake yoipa ni makumbilo yake.
Pakuti anyiimwe mdatanidwa ni Mnungu dala mkale afulu, ufulu wanu usidakhala ndande yochata makumbilo ya thupi, nambho mfunika mtumikilane kwa chikondi.
Uyo wavyala mkumbilo la jhiko, siwakolole mmenemo chiwanangiko, nambho wakavyala pa chizimu wa Mnungu, siwakolole umoyo wa muyaya kuchokela kwa mzimu wa Mnungu.
Chezelani ni kupembhela kuti msadalowa mu mayeselo. Mtima ufuna kuchita yayo yafunika, nambho thupi lilibe mbhavu."
Achabale nikamba chimwechi, chijha chachitidwa kwa thupi ni mwazi sichikhoza kulunjana ni Ufumu wa Mnungu, niicho chiwanangika sichikhoza kukhala chosawanangike.