Pular para o conteúdo
Publicidade

Encorajamento

Por Bíblia Online

O encorajamento é uma das vocações mais lindas do cristão. A Bíblia transborda de palavras de ânimo: não temas, levanta-te, Eu sou contigo. Deus nos encoraja para encorajarmos outros.

Não temas

Deus diz repetidamente: não temas, Eu sou contigo. Ele fortalece, sustenta e caminha ao nosso lado em cada desafio.

Deus está conosco

Se Deus é por nós, quem será contra nós? Tudo posso naquele que me fortalece. Ele nos encoraja pela sua presença.

Chikondi cha Mnungu kupitila Kilisito Yesu

Kuchokana ni yameneyo, sitikambe chiyani? Ngati Mnungu wali pamojhi ni ife, yani wakoza kutichucha?

Pakuti simdalandile Mzimu wakukuchitani anyiimwe akapolo ni kukupachani mandha, nambho mwalandila Mzimu wakukuchitani anyiimwe wana a Mnungu, ni mwa Mzimu umeneo ife timtana Mnungu, "Aba" Mate yake, "Tate!"

Tifunika kwa thangatila wina pakuchita vabwino, ni kwachita aime kwa Ambuye.

Mnungu nde uyo watithila mtima ni nde uyo watichita tilimbe mtima. Chipano nipembha kuti, wachitichite mukhale kwa maganizo yamojhi, ndande mwachata Ambuye Yesu.

Pakuti nikhumbila kupunda kukuonani, kuti nikhoze kukutangatilani kupata mbhaso ya mzimu Woyela ya kukulimbichani chikhulupi chanu. Ndiipo anyiimwe pamojhi ni ine, titilane mtima kuti chikhulupi chatu chiime bwino.

Nikhoza kuchita vindhu vonjhe mwa iye wanipacha mbhavu.

Nikhulupila kuti Mnungu waiyamba njhito ii ya bwino mmitima mwanu siwaiendeleze mbaka ikwanile musiku ijha ya Kilisito Yesu.

Chimwecho mundhu waliyonjhe wakalunjana ni Kilisito, wakhala mundhu wa chipano, yakale yatha, yakhala yachipano.

Kukhala kwa chikhulupi

Chimwecho, sitikufa mtima ata ngati matupi yathu yalema ni kuzeeka, nambho mkati tichitidwa kukhala achipano kila siku.

Kulaga kwathu nikochepa, ni kwa ndhawi yochepape, nambho kutikonjekela ulemelelo wa muyaya uwo upitilila vindhu vonjhe ivo tivilindilila.

Ndiipo ife tili ni kuikila uku tilingana ni miphika dala ijhiwike kuti mbhavu imeneyo yaikulu ichoka kwa Mnungu asati kwatu tachinawefe. Tilaga kila mtundu, nambho sitiyomwechedwa, tikhala ni mandha nambho sitikufa mtima, tivutika, nambho Mnungu siwatileka, tigwechedwa panjhi nambho sitidimbika. Siku zonjhe afuna kutipa ngati umo adamphela Yesu, dala umoyo wa Yesu uonekele mmatupi yathu. Ife tili amoyo sikuzonjhe tachochedwa timwalile ndande ya Yesu, dala umoyo wa Yesu uonekele mmatupi yathu yayo yamwalila.

Kilisito wavanicha wandhu ni Mnungu

Ife tijhiwa ubwino wa kumulambila Ambuye, chimwecho tijhitahidi kwakoka wandhu wina. Mnungu watijhiwa mokwanila, nane nikhulupilila kuti mtijhiwanjho bwinobwino. Sitifuna kujhikweza kwanu, nambho tifuna kukupachani ndande zathu zoona ufulu kwanu, dala mkhoze kwa yangha yao ajhidamila vichito vawo va kubwalo kupunda kusiyana ni umo ali mmitima yao. Ata ngati tioneka ozelezeka, imeneyo ndande ya Mnungu, ngati tili olungwamika, imeneyo ndande yanu. Chikondi cha Kilisito chitichogoza, ndande tikhulupilila kuti mundhu mmojhi wadafa ndande ya onjhe, chimwecho onjhe agwilizana ni nyifa yake. Wadafa ndande yaonjhe, dala kuti anyiyao akhala moyo asadakhala moyo kwa ndande yao achinawene, nambho akhale moyo ndande ya uyo wadafa, ni kuhyukichidwa ndande yao.

Chimwecho, kuyambila chipano sitimlamula mundhu waliyonjhe kwa kumpenya, ngati umo amjhiwila wandhu. Ingakhale ndhawi ina tidampenya Kilisito ngati mundhu, chipano sitichitanjho chimwecho. Chimwecho mundhu waliyonjhe wakalunjana ni Kilisito, wakhala mundhu wa chipano, yakale yatha, yakhala yachipano. Yaya yonjhe yachitika ni Mnungu, kutivanicha ife ni iye kwa kupitila Kilisito, nikutipacha njhito ya kwavanichana wandhu ni iye. Ndekuti Mnungu wadali mkati mwa Kilisito niwalivanicha jhiko la panjhi ni iye, popande kuwelenga machimo yao. Iye watipacha ife nghani ya Uthenga wa kwapatanicha wandhu alunjane ni iye. Ife ni athenga a Kilisito, Mnungu nayo watitumila ife kukupepezani anyiimwe. Ichi ndeicho Kilisito watifuna ife kukupembhani anyiimwe mchichite, mvanichidwe ni Mnungu. Kilisito wadalibe chimo, nambho Mnungu wadamchita wakhale ngati wamachimo ndande yathu, dala ife kwa kulunjana naye tikhale wovomelezeka kwa Mnungu.

Ikakhala mundhu wali ni mtima ochocha, Mnungu siwalandile chijha wakhoza kuchocha, asati kopenya icho walibe.

Poolo wamuyamika Mnungu

Watamandidwe Mnungu ni Tate wa Mbuye wathu Yesu Kilisito, Tate uyo wali ni lisungu ni Mnungu watithila mtima. Iye watithila mtima pa kulaga kwathu konjhe, dala nafe tathile mtima wina yawo alaga, pakwathila mtima ngati umo Mnungu watithilila ife mtima.

Ânimo nas lutas

No mundo tereis aflições, mas tende bom ânimo — Eu venci o mundo. O Senhor é refúgio seguro em toda tribulação.

Nakukambilani vindhu ivi dala mukhale ni mtendele pakulunjana niine. Simvutike pajhiko, nambho jhipacheni mtima! Ine nazikhoza mbhavu zoipa za jhiko lino!"

Nakukambilani vindhu ivi dala mukhale ni mtendele pakulunjana niine. Simvutike pajhiko, nambho jhipacheni mtima! Ine nazikhoza mbhavu zoipa za jhiko lino!"

"Mtendele nikusiilani, nikupachani mtendele wanga. Yetu nikupachani osati ngati umo likupachilani jhiko la panjhi. Simudakhaikila mumtima ni simdaopa.

"Mtendele nikusiilani, nikupachani mtendele wanga. Yetu nikupachani osati ngati umo likupachilani jhiko la panjhi. Simudakhaikila mumtima ni simdaopa.

Promessas de conforto

Vinde a mim os cansados e sobrecarregados. Lança sobre Ele tuas ansiedades, pois Ele cuida de ti.

"Majhani kwa ine, mwaonjhe mchauchika ni kuvutika ni makatundu yolemela, ine sinikuchiteni mpumulile.

Msadaopa yawo akhoza kukuphani anyiimwe, nambho sakhoza kuyomwecha mizimu yanu. Nambho muopeni yujha wakhoza kuyomwecha thupi pamojhi ni mzimu mumoto wa muyaya.

Encorajar uns aos outros

Encorajai-vos mutuamente e edificai-vos uns aos outros. Não desanimemos — a bondade do Senhor é nova a cada manhã.

Chimwecho achabale wanga, imani nganganga msada tingizika. Mpunde kuichita njhito ya Ambuye, mate mjhiwa njhito ya Ambuye siitaika chajhe.

Mawu yomalizila

Khalani maso, imani nganganga muchikhulupi, msadaopa, ni mkhale ni mbhavu.

Mawu yomalizila

Khalani maso, imani nganganga muchikhulupi, msadaopa, ni mkhale ni mbhavu.

Yesu wadaakambila, "Nichateni, nane sinikuyaluzeni mukhale owapeleka wandhu kwa ine, ngati umo mmavuwila njhomba." Pampajha adavisia vilepa vao nikumchata.

Deus chama pelo nome

Ao longo da Bíblia, Deus chamou seus servos pelo nome — Abraão, Moisés, Samuel, Paulo — encorajando cada um pessoalmente.

Kudali mundhu wokhulupilila mmojhi mu mujhi wa Damasika uyo wamatanidwa Ananiya. Iye wadatanidwa ni Ambuye mumasombhenya, "Ananiya!" Iye wadayangha,

"Ine pano Ambuye!"

Maliya wadayangha, "Ine ni mbowa wa Ambuye, mawu yaya yachitike ngati umo mwakambila." Ndiipo mtumiki wa kumwamba wadachokapo.

Bwanji, njhwala zisano sizigulichidwa kwa mtengo waung’ono kupunda? Nambho, pamaso pa Mnungu siiwalika ata njhwala imojhi. Zenedi, ata machichi ya mmitu yanu, yawelengedwa. Chipano, msadaopa, anyiimwe nde muli ni phindu kupunda kupitilila njhwala!"

Seja o primeiro