Espírito
O espírito humano é a parte mais profunda do nosso ser — onde Deus habita, onde a fé se ancora e de onde brota a verdadeira adoração. A Bíblia nos chama a viver pelo Espírito.
A natureza do espírito
O espírito está pronto, mas a carne é fraca. A batalha entre carne e espírito é constante e exige vigilância.
Chezelani ni kupembhela kuti msadalowa mu mayeselo. Mtima ufuna kuchita yayo yafunika, nambho thupi lilibe mbhavu."
Chikondwelo cha zene
"Ali ni mwawi wajha ajhiwa kuti amfuna Mnungu
pakuti ufumu wa kumwamba ni wao."
Pakuti makhumbolo yoipa yachuchana ni makhumbilo ya Mzimu wa Mnungu, nayo Mzimu wa Mnungu siwakhumbila vindhu voipa. Vindhu vimenevo vichuchana, ndande imeneyo simkhoza kuchita yayo mfuna.
Kuchogozedwa ni Mzimu wa Mnungu
Chipano nikamba chimwechi, ukhalo wanu uchogozedwe ni Mzimu wa Mnungu, mkachita chimwecho simuchatanjho makumbilo yoipa.
Nambho ivo vichokela ukachogozedwa ni Mzimu wa Mnungu ni chikondi, kukondwela, mtendele, kulimba mtima, ubwino, kutangatila wina ni kukhulupilika, wojhichicha ni kujhilamula umwene. Palibe thauko ilo lichogoza kuvichucha vindhu vimenevo.
Tikakhala kwa mthandizo wa Mzimu wa Mnungu, ifunika chinchijha tichate uchogolelo wake.
Maganizo yayo yachogozedwa ni thupi yapeleka nyifa, nambho maganizo yayo yachogozedwa ni Mzimu yapeleka umoyo ni mtendele.
O Espírito de Deus em nós
Vosso corpo é templo do Espírito Santo. Deus fortalece com poder no homem interior pelo seu Espírito.
Simujhiwa kuti mathupi yanu ni nyumba ya Mzimu Wamnungu, uwo ukhala mkati mwanu ni uwo mwapachidwa ni Mnungu? Mathupi yanu osati yanu mwachinawene nambho ni ya Mnungu, pakuti mdaghulidwa kwa mtengo wa ukulu. Tumilani matupi yanu kwa ulemelelo wa Mnungu.
Nambho iye walunjana ni Ambuye wakhala mzimu umojhi ni Ambuye.
Palibe mundhu uyo wajhiwa maganizo ya mundhu mwina. Chimchijha mzimu wokha ulimkati nde ujhiwa maganizo ya mundhu mmeneyo, chimwecho ndeumo ili ata kwa Mnungu, Mzimu wokha wa Mnungu nde ujhiwa maganizo ya Mnungu.
Nichite chiyani, ndiipo sinipembhe kwa mzimu wanga, sinipembhenjho kwa njelu yanga, niimbe kwa mzimu wanga, niimbenjho kwa njelu yanga.
Nimpembha Mnungu, wakupacheni ngati umo kuli kuchuluka kwa ulemelelo wake, wakupacheni mbhavu za mzimu wake, ni mbhavu mkati mwanu yoima nganganga, dala Kilisito wakhale mkati mwanu kwa njila ya kumkhulupilila. Nimpembha Mnungu yonjhe yayo muyachita yachoke muchikondi cha zene,
Niyendekela kumpembha Mnungu wa Ambuye wathu Yesu Kilisito, Atate aulemelelo, akupachenu Mzimu wao uwo siukuchiteni mkhale woyela ni kukuvunukulilani kumjhiwa Mnungu.
Pakuti simdalandile Mzimu wakukuchitani anyiimwe akapolo ni kukupachani mandha, nambho mwalandila Mzimu wakukuchitani anyiimwe wana a Mnungu, ni mwa Mzimu umeneo ife timtana Mnungu, "Aba" Mate yake, "Tate!" Nawo Mzimu wene ulangiza mkati mwa mitima yathu, kuti ife ni wana a Mnungu.
Nawo Mzimu wene ulangiza mkati mwa mitima yathu, kuti ife ni wana a Mnungu.
Pakuti simdalandile Mzimu wakukuchitani anyiimwe akapolo ni kukupachani mandha, nambho mwalandila Mzimu wakukuchitani anyiimwe wana a Mnungu, ni mwa Mzimu umeneo ife timtana Mnungu, "Aba" Mate yake, "Tate!"
Nambho ngati Kilisito wali mkati mwanu, matupi yanu siyamwalile ndande ya machimo, nambho Mizimu yanu yamoyo ndande mwachitidwa kukhala Amnungu.
Wonjhe achogozedwa ni Mzimu wa Mnungu ni wana wa Amnungu.
Ife tilibe mbhavu nambho Mzimu wa Amnungu utithangatila. Pakuti sitijhiwa umo ifunika kupembela, nambho Mzimu wene utipembhela kwa Mnungu kwa kubuula ukosikukambika.
Msidakhala alesi kuchita jhito ya Mnungu, mchite njhito imeneyo kwa mtima onjhe ni kumtumikila Mnungu.
Mnungu wa chikhulupi uyo wakuthilani anyiimwe mtima ni mtendele pa kumkhulupilila, mpate kujhazidwa ni chikhululupilo chachikulu kwa mbhavu za mzimu wa Mnungu.
Vida no Espírito
Deus é Espírito e importa que os que o adoram o adorem em espírito e em verdade. O Espírito vivifica e transforma.
Amnungu ni Mzimu, ni wonjhe amlambila afunika kumlambila muchizimu ni zene."
Ndhawi ikujha, ni chipano ilipo, wandhu azene yapo samlambile Mnungu kwa kuchogozedwa ni Mzimu ni zene. Amnungu waafuna anyiyao alambila mtundu uwu. Amnungu ni Mzimu, ni wonjhe amlambila afunika kumlambila muchizimu ni zene."
Chimwecho, ife yao nghope zathu sizidavinikilidwe, tiuona ulemelelo wa Ambuye, ngati mukiyoo. Njhito ya Mzimu wa Ambuye iting’anamucha ife tilingane kupunda ni chifani chake kuchoka ulemelelo mbaka ulemelelo waukulu kupunda.
Ndipo, okondedwa wanga, pakuti tili ni yayo Mnungu watikambila kuti siwatipache, chimwecho tijhieleche mmitima yathu ni chilichonjhe icho chikhoza kudecha matupi yathu ni mizimu yathu, tikhale oyela ni kumlambila Mnungu.
pakuti, nijhiwa kwa kupembha kwanu, ni kutangatilidwa ni Mzimu wa Yesu Kilisito, yajha yadanipata ine siyang’anamuke kukhala uomboli.
Mwachitilidwa ubwino wa Ambuye Yesu Kilisito pamojhi ni mzimu wanu.
Promessas do Espírito
Derramarei o meu Espírito sobre toda a carne. O Espírito revela, guia e capacita os filhos de Deus.
Cuidar do espírito
Cria em mim um coração puro e renova dentro de mim um espírito reto. O espírito quebrantado Deus não rejeita.
Chipano ngati anyiimwe, yawo muli wolakwa, mujhiwa kwapacha wana wanu vindhu vabwino, zenedi Atate wanu wakumwamba sayendekele kupunda kwapacha Mzimu Woyela yawo ampembha."
Kudatulukila malilime ya moto yayo yadagawika ni kukhala pamwamba pa kila mmojhi wawo. Wandhu wonjhe adajhazidwa ni Mzimu Woyela, adayamba kukamba mikambo ya chilendo, ngati umo wadafunila Mzimu Woyela.