O marido
A Bíblia define o papel do marido com clareza: amar a esposa como Cristo amou a Igreja, ser fiel, protetor e líder servo no lar.
Amar como Cristo amou
Maridos, amai vossas mulheres como Cristo amou a Igreja e se entregou por ela. O amor do marido deve ser sacrificial e incondicional.
Anyiimwe wachimuna, mjhakonda achakazanu ngati Kilisito umo wadalikondela gulu lake, wadajhichocha njhembe ndande yawo,
Chimwecho wachimuna afunika kwakonda achakazao ngati matupi yawo. Uyo wamkonda mkazake mmeneyo wajhikonda mwene.
Chimwecho wachimuna afunika kwakonda achakazao ngati matupi yawo. Uyo wamkonda mkazake mmeneyo wajhikonda mwene. Palibe mundhu uyo waliipila thupi lake, nambho walidyecha ni kuliveka. Nde umo Kilisito walisungila gulu lake,
Nambho kila wammuna ifunika wamkonde mkazake ngati mwene wake ni wamkazi wafunika kumsamala mmunake.
Chimwecho, usiyeni unami. Kila mmojhi wafunika wamkambile mnjake uzene, ndande kila mmojhi ni chiwalo cha Kilisito. Mkakwiya, mbhwai yanu siidakuchitichani mchite machimo, ni simdalongeza ni mbhwai siku la mbhumbhu mbaka yapo jhuwa yapo libila, dala simudampacha Satana malo. Uyo wakuba, siwadabanjho, nambho wayambe kuchita njhito yabwino kwa manja yake, dala wakhale ni chindhu cha kumthangatila osauka. Simudakamba mawu yoipa, nambho mawu yanu yajhikhala ya kwathangatila wina kuchokana ni icho afuna, dala yathangatile yawo akuvelani. Simudamdandaulicha Mzimu wa Mnungu, pakuti Mzimu umeneo ni chizindikilo cha Mnungu kwanu kuti anyiimwe ni wandhu wake, ni uchimikizo ndande ya siku la uomboli. Chimwecho siyani kukhala ni dungulila, ipilo, mbhwai, pokoso ni matukwano ni msiye kila mtundu wa voipa. Mkhale ni mtima wa bwino ni kulengelana lisungu, kila mmojhi wamlekelele mnjake ngati Mnungu umo wakulekelelani anyiimwe kwa kupitila ya Kilisito.
Fidelidade conjugal
O casamento é honroso e o leito conjugal é santo. O marido deve ser fiel à esposa da sua juventude em pensamento e ação.
Nambho ine nikukambilani kuti uyo siwampenye wamkazi kwa kumkhumbila wathochita chigololo mumtima mwake.
Nambho ine nikukambilani mundhu waliyonjhe uyo siwamsiye mkazake kwa ndande yaliyonjhe ijha ni osati kwa ndande ya chigololo wamchita mkazake kukhala wachigololo, ni wammuna waliyonjhe uyo siwamkwate wamkazi uyo wasiidwa nayo wachita chigololo."
Chimwecho, anyiiwo osati awilinjho, nambho thupi limojhi. Icho wachilunjanicha Mnungu, mundhu siwadachisiyanicha."
Wammuna wachite umo ifunikila kwa mkazake, ni wamkazi wachite umo ifunikila kwa mmunake, ni kila mmojhi wamkwaniliche mnjake icho chifunika. Wamkazi walibe lamulo pamwamba pa thupi lake, nambho mmunake wali nilamulo pamwamba pa thupi la mkazake, chinchijha wammuna nayonjho walibe lamulo pamwamba pathupi lake, nambho mkazake wali nilamulo pa mwamba pathupi la mmunake.
Msadamanana nambho ikakhala mwavomelezana dala mpheze ndhawi ya mapembhelo, ndiipo mbwelelenjho ili Mdani wa Mnungu siwadapheza kukuikani mmayeso ndande ya kulepela kuchekeleza mafuno yanu.
Nambho kwa anyiwajha akwata nili ni lamulo. Wamkazi siwadasiyana ni mmunake, nambho ikakhala wamkazi wasiyana nimmunake, siwada kwatiwa, kapina wabwelelane ni mmunake, ni wammuna siwadalemba kalata ya kumsiya mkazake.
Nambho kwa wina, ine nikukambilani osati Ambuye akamba, ngati wammuna wali ni wamkazi, siwada khulupilile, ni wamkazi wavomela kukhala nayo siwadamsiya.
Chithaweni chigololo. Machimo yina yonjhe wachita mundhu wachita kubwalo kwa thupi lake, nambho mundhu uyo wachita chigololo wachita mkhati mwathupi lake mwene wake.
Convivência com sabedoria
O marido sábio vive com a esposa com entendimento, dando-lhe honra como co-herdeira da graça. A união conjugal reflete Cristo e a Igreja.
Msada chita chindhu chalichonjhe kwandane yanu kapina kujidamila, ila kwa kunyenyekela kila mmojhi wamuone mnjake wamate kupita iye. Kila mmojhi siwadajhipenya kupata kwake mwenepe, nambho wapenye kupata kwa mnjake.
Poolo wakaniza wandhu kulunjana ni wandhu samkhulupilila Mnungu
Msada gwilizana ni wandhu osakhulupilile Mnungu. Bwanji ubwino ni kuipa vikoza kukhala pamojhi? Dangalila ni mdima vikhoza bwanji kukhala pamojhi?
Uyo wali ni chikondi waembekeza, wathangatila, uyo wali nichikondi walibe njhanje, walibe dama, kapina kujhiona, uyo wali ni chikondi siwachepa ulemu, uyo wali ni chikondi siwafuna vindhu va kumthangatila mwene, kapina mbhwai za msanga, siwasunga chikumbukilo cha voipa, mundhu wa chikondi siwakondwela voipa, nambho chikondwela uzene. Mundhu wachikondi wapilila yonjhe, mundhu wa chikondi wakhulupila wina, mundhu wa chikondi waembekeza, ni siwalepela.