Pão
O pão é símbolo central na Bíblia: do maná no deserto ao pão da vida — Jesus. A Escritura usa o pão para ensinar sobre provisão divina, comunhão e dependência espiritual.
O maná do céu
Deus alimentou Israel no deserto com pão do céu. O maná era diário, fiel e suficiente — retrato da provisão constante de Deus.
O pão da vida
Jesus declarou: 'Eu sou o pão da vida.' Quem vem a Ele nunca terá fome, e quem nele crê jamais terá sede. Ele é o sustento eterno.
Ndiipo Yesu wadakambila, "Zene nikukambilani, osati Musa uyo wadakupachani chakudya kuchoka kumwamba, nambho Atate wanga nde yao akupachani chakudya cha uzene kuchoka kumwamba. Pakuti bumunda la Amnungu nde uyo wachika kuchoka kumwamba ni kwapacha umoyo wandhu a jhiko la panjhi."
Ndiipo adamkambila, "Tipache chakudya chimenelo siku zonjhe."
Chimwecho wadaakambila, "Ine nde chakudya cha umoyo. Uyo wakujha kwanga siwaona njala ni uyo wanikhulupilila siwaona lujho muyaya.
Ine nde chakudya cha umoyo. Azee wanu adadya chakudya icho chitanidwa mana ku phululu, nambho adamwalila. Nambho chino nde chakudya icho chichoka kumwamba, kuti waliyonjhe uyo wakudya siwadamwalila. Ine nde chakudya chili cha moyo icho chachika kuchoka kumwamba. Mundhu waliyonjhe uyo siwadye chakudya ichi siwakhale moyo muyaya. Ni chakudya icho sinimpache, nde thupi langa ilo nichocha ndande ya wandhu ajhiko la panjhi."
Yesu wadamuyangha, "Yalembedwa, ‘Mundhu siwakhala wa moyo kwa bumundape, Nambho kwa kila malembo yoyela yakambidwa ni Mnungu.’"
Partilha e comunhão
O partir do pão une o corpo de Cristo. Na Ceia, na generosidade e na partilha, expressamos a comunhão com Deus e uns com os outros.
Ndiipo, wadatenga bumunda, wadayamika, ni kuubandhula, wadapacha atumwi ni kukamba, "Ili ni thupi langa ilo lichochedwa ndande ya anyiimwe. Mjichite chimwechi ponikumbukila ine."
Pakuti kila yapo simujhidya bumunda ili ni kumwa mchikho ichi, muuzila wina Ambuye adafa ndande yanu mbaka yapo siwajhe.
Chikho chijha cha mwawi tichitumila kwa chakudya cha Mbuye, sitigwilizana ni mwazi wa Kilisito? Ni yapo tibandhula lijha bumunda, sitigwilizana ni thupi la Kilisito? Pakuti bumunda nilimojhi, ife taonjhe tili ambili tili thupi limojhi, taonjhe tililandila bumunda limwelo limojhi.
Nambho anyiimwe pembhelani chimwechi,
‘Atate wathu yawo muli kumwamba,
Jhina lanu likwezedwe.
Ufumu wanu ujhe.
Ilo mlifuna lichitike pa jhiko lichitike ngati umo lichitikila kumwamba.
Mtipache lelo chakudya chatu ngati umo mtipachila.
Nambho Yesu wadaakambila, "Mwachinawene wake mwapache chakudya." Ni anyiiyo adamfunjha, "Bwanji, tipite kugula mabumunda ya dinali miyambili ni kwapacha wandhu adye?" Yesu waadafunjha, "Mli ni mabumunda yangati? Pitani mkapenye, mkaiwelenge." Yapo adawelenga, adamkambila, "Yalipo mabumunda yasano ni njhomba ziwili."
Ndiipo, Yesu wadaakambila oyaluzidwa wake, waakambile wandhu akhale magulu mgulu pamachamba yayawisi. Chimwecho adakhala magulu ya wandhu miya ni ya wandhu amsini. Ndiipo, Yesu wadayatenga yajha mabumunda yasano ni zijha njhomba ziwili, wadapenya kumwamba, wadamuyamika Mnungu, ndiipo wadayadula yajha mabumunda. Wadaapacha oyaluzidwa wake kuti wagawile wandhu. Chinchijha wadagawila wandhu zijha njhomba ziwili. Wandhu wonjhe adadya ni kukhuta. Ndiipo oyaluzidwa wake adatondola vidufya va mabumunda ni njhomba ivo vidakhalila, ni adajhaza miseche khumi ni iwili.
Provisão divina
O justo não é desamparado e seus descendentes não mendigam pão. Deus provê com fidelidade o alimento de cada dia.
Amila ya Afalisayo ni Asadukayo
Oyaluzidwa wake yapo adayomboka kuchijya la nyanja, adazindikila kuti aiwala kutenga mabumunda. Yesu wadaakambila, "Khalani maso ni mjhipenyelele ni amila ya Afalisayo ni Asadukayo."
Ndiipo oyaluzidwa adayamba kukambilana achinawene kwa achinawene, "Wakamba chimwechi ndande sitidatenge mabumunda."
Yesu wadayajhiwa yayo amachuchana, wadaakambila, "Imwe, wandhu mukhulupilila pang’ono! Bwanji muchuchana mwachinawene ndande yosatenga mabumunda? Bwanji, mkalipe osajhiwe? Bwanji, simukumbukila mabunda yasano yajha nidapacha wandhu elufu zisano? Bwanji, mdajhaza miseche ingati ya vijha vokhalila? Kapina mabumunda saba yajha mudagaawila wandhu elufu zinayi, chiwelengelo cha miseche ingati mudakusa? Bwanji, simudajhiwa kuti sinimakambe nghani za mabumunda? Jhipenyeleleni ni amila ya Afalisayo ni Asadukayo."
Pamenepo oyaluzidwa wake adajhiwa kuti siwadakambile ajhipenyelele ndande ya amila ya mabumunda, nambho ajhipenyelele ni mayaluzo ya Afalisayo ni Asadukayo.