Pular para o conteúdo
Publicidade

Resultados da busca por "esperança"

27 resultados encontrados

  1. Provérbios 13

    Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
    Capítulo 13
    Mostrando versículos 8–14 de 25

    8Chuma cha munthu wolemera chitha kuwombola moyo wake,koma munthu wosauka amamva chidzudzulo.

    12Chinthu chochiyembekezera chikalephereka chimalefula mtima,koma chinthu chochilakalaka chikachitikadi chimakhala ngati mtengo wamoyo.

    14Malangizo a munthu wanzeru ali ngati kasupe wamoyo;amathandiza munthu kuti asakondwe mu msampha wa imfa.

  2. Romanos 12

    Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
    Capítulo 12
    Mostrando versículos 9–15 de 21

    9Chikondi chikhale chopanda chinyengo. Dana nacho choyipa; gwiritsitsa chabwino.

    12Kondwerani mʼchiyembekezo, pirirani mʼmasautso ndiponso khulupirikani mʼpemphero.

    15Kondwani pamodzi ndi amene akukondwa ndipo lirani ndi amene akulira.

  3. Salmos 123

    Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
    Capítulo 123
    Mostrando versículos 1–4 de 4

    1Ndikweza maso anga kwa Inu,kwa Inu amene mumakhala kumwamba.

    3Mutichitire chifundo, Inu Yehova mutichitire chifundo,pakuti tapirira chitonzo chachikulu.

    4Ife tapirira mnyozo wambiri kuchokera kwa anthu odzikuza,chitonzo chachikulu kuchokera kwa anthu onyada.

  4. Provérbios 10

    Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
    Capítulo 10
    Mostrando versículos 15–28 de 32

    15Chuma cha munthu wolemerandiye chitetezo chake; koma umphawi ndiye chiwonongeko cha osauka.

    17Wosamalira malangizo amayenda mʼnjira ya moyo,koma wonyoza chidzudzulo amasochera.

    28Chiyembekezo cha olungama chimapatsa chimwemwe,koma chiyembekezo cha anthu ochimwa chidzafera mʼmazira.

  5. Salmos 119

    Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
    Capítulo 119
    Mostrando versículos 81–147 de 176

    81Moyo wanga wafowoka ndi kufunafuna chipulumutso chanu,koma chiyembekezo changa chili mʼmawu anu.

    88Sungani moyo wanga molingana ndi chikondi chanu chosasinthika,ndipo ndidzamvera umboni wa pakamwa panu.Lamedi

    147Ndimadzuka tambala asanalire kuti ndipemphe thandizo;chiyembekezo changa chili mʼmawu anu.

  6. Salmos 150

    Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
    Capítulo 150
    Mostrando versículos 3–6 de 6

    3Mutamandeni poyimba malipenga,mutamandeni ndi pangwe ndi zeze.

    4Mutamandeni ndi matambolini ndi kuvina,mutamandeni ndi zingwe ndi zitoliro.

    6Chamoyo chilichonse chopuma chitamande Yehova.Tamandani Yehova.

  7. Salmos 3

    Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
    Capítulo 3
    Mostrando versículos 2–8 de 8

    2Ambiri akunena za ine kuti,"Mulungu sadzamupulumutsa."Sela

    4Kwa Yehova, Ine ndilira mofuwulandipo Iye amandiyankha kuchokera ku phiri lake loyera.Sela

    8Chipulumutso chimachokera kwa Yehova.Madalitso akhale pa anthu anu.Sela

Léxico (correspondência exata) Semântico (correspondência relacionada) Versículos omitidos Contexto do capítulo