Superação
Superar desafios, dificuldades e tentações faz parte da caminhada cristã. A Bíblia nos garante que, em Cristo, somos mais que vencedores em todas as circunstâncias.
Vitória em Cristo
Jesus já venceu o mundo. Nele temos coragem, paz e a certeza de que nenhuma adversidade poderá nos derrotar definitivamente.
Nakukambilani vindhu ivi dala mukhale ni mtendele pakulunjana niine. Simvutike pajhiko, nambho jhipacheni mtima! Ine nazikhoza mbhavu zoipa za jhiko lino!"
Nakukambilani vindhu ivi dala mukhale ni mtendele pakulunjana niine. Simvutike pajhiko, nambho jhipacheni mtima! Ine nazikhoza mbhavu zoipa za jhiko lino!"
Nambho pa vindhu vimenevo vonjhe, tikhoza ndande tithangatilidwa ni Klisito uyo watikonda.
Nambho wayamikidwe Mnungu, iye watipacha kukhoza kwa kupitila Yesu Kilisito!
Nambho wayamikidwe Mnungu, iye watipacha kukhoza kwa kupitila Yesu Kilisito!
Superando o mal com o bem
O cristão vence o mal não com violência, mas com o bem. O amor, a fé e a perseverança são as armas da superação.
Siudavomela kulepela ni voipa, nambho ukukhoze kuipa kwa ubwino.
Siudavomela kulepela ni voipa, nambho ukukhoze kuipa kwa ubwino.
Dangalila limenelo liwala mumdima, ni mdima siudalikhoze kulithima dangalila limenelo kuti lisawale.
Nambho wayamikidwe Mnungu uyo watichogoza kukhoza kwa kulunjana ni Kilisito. Iye watichita tieneze uzene wa Kilisito ngati mnunghilo wa bwino kila kumalo.
Mkamlekelela mundhu, nanenjho namlekelela. Pakuti yapo nilekelela, ngati nili nikandhu kalikonjhe komlekelela, nimlekelela uku Kilisito niwachimikiza, dala sitidamsiya Mdani wa Mnungu watinyenge, pakuti maganizo yake tiyajhiwa umo yali.
Força e coragem divina
Deus é nosso escudo e fortaleza. Quando o medo tenta nos paralisar, a presença do Senhor nos fortalece e nos encoraja a prosseguir.
Nikhoza kuchita vindhu vonjhe mwa iye wanipacha mbhavu.
Resistindo a tentação
A armadura de Deus nos protege contra as investidas do mal. Resistir ao diabo, vigiar e orar são essenciais para a superação espiritual.
Mathelo, niikufunani mukhale nganganga pa kulunjana ni Ambuye ni kwa kukhozechedwa kwa mbhavu zake. Valani vida vonjhe va Mnungu, mkhoze kuchekeleza misambha ya Satana. Nghondo yathu asati kubulana ni wandhu, nambho kubulana ni magulu ya viwanda mujhiko la chizimu, tibulana ni alamuli, afumu ni ambhavu za yawo alamulila jhiko lino la chizimu. Chimwecho, valani vida ivo wakupachani Mnungu, mkhoze kulimbana pa siku la mavuto, ni mkabulana mbaka pothela simuendekele kukhala nganganga.
Chipano, imani nganganga, muli wojhimanga zene ngati lamba muchiuno mwanu, kuvomelezeka kukhale ngati chivalo cho jhikengelela pamtima, mkhale tayali kulalikila Uthenga Wabwino wa mtendele ngati vilato myendo mwanu. Kupitilila yonjhe, chikhulupi chikhale chitetezo mmanja mwanu, chikhoze kizithima misonga ya moto ya satana. Ulandileni uomboli ngati chisoti cha chichulo, ngati upanga wa Mzimu uwo uli mawu la Mnungu.
Mudayaluzidwa muvisiye vichito vanu voipa ivo madavichita kale, ngati mujha mundhu wavulila njalu ni kuisiya, vichito ivo vimawanangidwa ni khumbilo launami. Mmizimu mwanu ni mmaganizo yanu mving’anamule vikhale va chipano. Mkhale ni umoyo wa chipano, ngati umo mmungu wadakuumbani, mlingane niiye uku muli ovomelezeka kupunda ni kukhala umo ifunukila.
Mkakwiya, mbhwai yanu siidakuchitichani mchite machimo, ni simdalongeza ni mbhwai siku la mbhumbhu mbaka yapo jhuwa yapo libila, dala simudampacha Satana malo.
Mayeso yonjhe mwapata yakawaida kwa wandhu. Nambho Mnungu ni wokhulupilika siwavomela muyesedwe kupitilila yayo muyakhoza, nambho yapo muyesedwa, siwakupacheni njila yotulukila ili mukhoze kulimba mtima.
Perseverança até o fim
A corrida da fé exige perseverança. Devemos lançar fora todo peso e olhar para Jesus, o autor e consumador da nossa fé.
Niyani wakhoza kutiika patali nichikondi cha Kilisito? Bwanji ni kulaga, kapina mavuto, kapina njala, kapina kutedwa njhalu, kapina kuofyedwa kuphedwa?
Tijhiwa kuti pavindhu vonjhe, Mnungu wachita njhito pamojhi ni wonjhe wakonda pa kwapacha vabwino, yani wajha waadatana kuchokana ni dala lake.
Descanso e renovação
Jesus convida os cansados e sobrecarregados a descansar nele. Sua graça é suficiente para nos renovar em meio às tribulações.
"Majhani kwa ine, mwaonjhe mchauchika ni kuvutika ni makatundu yolemela, ine sinikuchiteni mpumulile.
Mate yake palibe chindhu icho sichikhozeka kwa Mnungu."
Iye wadaafunjha, "Bwanji mwagona? Ukani mupembhele kuti musadalowa mumayeso."
Yapo wadafika ku phili, wadaakambila, "Mjhipembhela kuti musadalowa mmayeso."
Yesu wadakambila ochatila wake kuti, Nikupachani ulamulilo wakuponda njoka ni chipilili ni mbhavu za adani wonjhe, sipakhalapo chindhu chilichonjhe icho sichikupwetekeni.
Ndiipo, wadaakambila, "Mchezelele ni mpembhele kuti simdayesedwa kuchita voipa. Anyiimwe mfuna kulimbila mtima mayeso nambho matupi yanu yalibe mbhavu."
Mujhiwa kuti mathupi yanu ni viwalo va thupi la Kilisito. Mukhoza kutenga chiwalo cha thupi la Kilisito ni kuchichita malo ya thupi la hule? Siikhozeka! Pakuti uyo walunjana ni hule wakhala thupi limojhi ni huleyo yalembedwa mmalembo ya Mnungu, "Nao awili akhala thupi limojhi." Nambho iye walunjana ni Ambuye wakhala mzimu umojhi ni Ambuye.
Chithaweni chigololo. Machimo yina yonjhe wachita mundhu wachita kubwalo kwa thupi lake, nambho mundhu uyo wachita chigololo wachita mkhati mwathupi lake mwene wake. Simujhiwa kuti mathupi yanu ni nyumba ya Mzimu Wamnungu, uwo ukhala mkati mwanu ni uwo mwapachidwa ni Mnungu? Mathupi yanu osati yanu mwachinawene nambho ni ya Mnungu, pakuti mdaghulidwa kwa mtengo wa ukulu. Tumilani matupi yanu kwa ulemelelo wa Mnungu.
Chipano nikamba chimwechi, ukhalo wanu uchogozedwe ni Mzimu wa Mnungu, mkachita chimwecho simuchatanjho makumbilo yoipa. Pakuti makhumbolo yoipa yachuchana ni makhumbilo ya Mzimu wa Mnungu, nayo Mzimu wa Mnungu siwakhumbila vindhu voipa. Vindhu vimenevo vichuchana, ndande imeneyo simkhoza kuchita yayo mfuna.