Pular para o conteúdo
Publicidade

Resultados da busca por "fé"

27 resultados encontrados

  1. 1 Coríntios 4

    Nyanja
    Capítulo 4
    Mostrando versículos 2–21 de 21

    2Chifunika kwa mtumiki ni kukhala wokhulupilila.

    15Ata ngati muli ni oyaluza khumi elfu mwa Kilisito, nambho muli ni atate amojhi. Pakuti ine nde navomela mwa Kilisito Yesu, kukupelekelani Uthenga Wabwino.

    21Anyiimwe msangha chiyani? Nijhe kwanu ni mkhwapulo, kapina nijhe mu chikondi ni mtima ofacha?

  2. Atos 25

    Nyanja
    Capítulo 25
    Mostrando versículos 2–22 de 27

    2Waakulu wa ajhukulu ni achogoleli Achiyahudi adajha kwa Fesito kumpacha mlandu wa Poolo. Adamkambila Fesito,

    16Nambho nidaayangha kuti mundhu yapo waphezeka mundhu uyo wali ni mlandu, ife Aloma tilibe mthethe wompeleka kwa wandhu wina kuti wagamulidwe. Poyamba wakomane ni yawo ampacha mlandu maso ni maso ni kupachita ndhawi yojhiteteya pa milandu iyo amushitaki.

    22Ndiipo Agilipa wadayangha, "Nidakakonda kumvechela mundhu mmeneyo namwene wake."Fesito wadayangha, "Siumvechele mawa."

  3. Romanos 9

    Nyanja
    Capítulo 9
    Mostrando versículos 16–32 de 33

    16Chimwecho yonjhe yakhulupila lisungu la Mnungu, nambho siya khulupilila bidii kapina kufuna kwa mundhu.

    20Nambho iwe mundhu iwe ni yani ata uyesa kumfunjha Mnungu? Bwanji mphika ukhoza kumfunjha uyo wauumba, "Ndande yanji waniumba chimwechi?"

    32Ndande ya kukhulupila vichito vao pambuyo pa kukhulupilila chikhulupi. Chimwecho, adajhikwala pamwamba pa mwala ujha "Ukwiicha."

  4. 1 Coríntios 12

    Nyanja
    Capítulo 12
    Mostrando versículos 8–20 de 31

    8Mzimu umpacha mundhu mmojhi mawu la ekima, ni mwina mawu lojhiwa umowakondela Mzimu mmeneyo.

    9Mzimu umweo umpacha mwina kukhoza kukhulupilila kwa kukulu, ni mwina wampacha kukhoza kulamicha odwala.

    20Uzene, nikuti kulini viwalo vambili nambho thupi limojhi.

  5. Atos 26

    Nyanja
    Capítulo 26
    Mostrando versículos 7–27 de 32

    7Ahadi iyo nde iyo mafuko yathu khumi ni yawili akhulupilila kuiona niikwanilichidwa, uku niyamtumikila Mnungu kwa mtima wonjhe usiku ni usana. Imwe amfumu ndande ya yaya, Ayahudi anyiiawa anipacha mlandu.

    8Ndande yanji waliyonjhe pakati panu waona kulimba kukhulupilila kuti Mnungu wakhoza kwaahyukicha wandhu yawo amwalila?

    27Mfumu Agilipa bwanji, mwaakhulupilila alosi? Nijhiwa kuti muyakhulupilila."

  6. 1 Coríntios 5

    Nyanja
    Capítulo 5
    Mostrando versículos 4–13 de 13

    4Mate yake, zene yapomsonghanika kumlambila Ambuye wathu Yesu nane nikhalapo pamojhi namwe mu mzimu ni kukhoza kwa Ambuye Yesu ukakhalapo.

    12Ili ni mate yanji kwalamula anyiwajha ali kubwalo? Achameneo Mnungu siwalamule. Nambho anyiimwe mufunika kulamula gulu lawandhu amkhulupilia Yesu, ngati umo malembo ya Mnungu yalembedwa, "Chocha wandhu oipa pakati panu."

    13Mnungu siwalamule anyiwajha ali kubwalo. Bwanji, anyiimwe simufuna kwalamula anyiyao ali mugulu la wandhu amkhulupilila Yesu? Ngati umo malembo ya Mnungu yalembedwa, "Chocha mundhu oipa pakati panu."

  7. Atos 23

    Nyanja
    Capítulo 23
    Mostrando versículos 13–28 de 35

    13Wandhu yawo adakambilana yameneyo adali wandhu wopitilila alobaini.

    25Ndiipo yujha wamkilu wa asikali wadalembela kalata Felikisi iyo idakamba kuti,

    28Nimafuna kujhiwa wali ni mlandu wanji, chimwecho nidapitanayo pachopgolo pa bwalo lawo lalikulu la milandu.

Léxico (correspondência exata) Semântico (correspondência relacionada) Versículos omitidos Contexto do capítulo