Pular para o conteúdo
Publicidade

Resultados da busca por "salvação"

78 resultados encontrados

  1. Lucas 12

    Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
    Capítulo 12
    Mostrando versículos 23–25 de 59

    23Moyo uposa chakudya, ndi thupi liposa chovala.

    24Taonani makwangwala: iwo safesa kapena kukolola, alibe nyumba zosungamo zinthu kapena nkhokwe; komabe, Mulungu amawadyetsa. Koposa kotani inu amene ndi ofunikira kuposa mbalame.

    25Ndi ndani wa inu akhoza kuwonjeza ora pa moyo wake chifukwa cha kudandaula?

  2. Isaías 61

    Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
    Capítulo 61
    Mostrando versículos 2–10 de 11

    2Wandituma kuti ndikalengeze nthawi imene Yehova adzapulumutsa anthu ake;za tsiku limene Yehova adzalanga adani a anthu ake.Wandituma kuti ndikatonthoze olira.

    3Wandituma kuti ndiwakonzere olira a ku Ziyoni,nkhata ya maluwa yokongolamʼmalo mwa phulusa,ndiwapatse mafuta achikondwereromʼmalo mwa kulira.Ndiwapatse chovala cha matamandomʼmalo mwa mtima wopsinjika.Ndipo iwo adzatchedwa mitengo ya thundu yamphamvu yachilungamo,yoyidzala Yehovakuti Iye mwini apezemo ulemerero wake.

    10Ine ndikusangalala kwambiri chifukwa cha Yehova;moyo wanga ukukondwera chifukwa cha Mulungu wanga.Pakuti Iye wandiveka zovala zachipulumutso,ndipo wandiveka mkanjo wachilungamo.Zili ngati mkwati wovala nkhata ya maluwa mʼkhosi mwake,ndiponso ngati mkwatibwi wovala mikanda yamtengowapatali.

  3. Êxodo 30

    Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
    Capítulo 30
    Mostrando versículos 1–26 de 38

    1Upange guwa lamatabwa amtengo wa mkesha lofukizirapo lubani.

    5Upange mizati yamtengo wa mkesha ndipo uyikute ndi golide.

    26Tsono uwagwiritse ntchito podzoza tenti ya msonkhano, Bokosi la Chipangano,

  4. Provérbios 16

    Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
    Capítulo 16
    Mostrando versículos 18–31 de 33

    18Kunyada kumafikitsa ku chiwonongeko,ndipo munthu wodzikuza adzagwa.

    25Pali njira ina yooneka ngati yowongoka kwa munthukoma kumatsiriziro kwake ndi imfa.

    31Imvi zili ngati chipewa chaufumu chaulemerero;munthu amazipeza akakhala moyo wolungama.

  5. 1 Crônicas 1

    Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
    Capítulo 1
    Mostrando versículos 21–26 de 54

    21Hadoramu, Uzali, Dikila

    22Obali, Abimaeli, Seba,

    26Serugi, Nahori, Tera

  6. Lucas 22

    Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
    Capítulo 22
    Mostrando versículos 1–43 de 71

    1Phwando la buledi wopanda yisiti lotchedwa Paska litayandikira,

    28Inu ndinu amene mwayima nane mʼmayesero.

    43Mngelo wochokera kumwamba anafika namulimbikitsa.

  7. Salmos 150

    Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
    Capítulo 150
    Mostrando versículos 1–6 de 6

    1Tamandani Yehova.Tamandani Mulungu mʼmalo ake opatulika;mutamandeni ku thambo lake lamphamvu.

    4Mutamandeni ndi matambolini ndi kuvina,mutamandeni ndi zingwe ndi zitoliro.

    6Chamoyo chilichonse chopuma chitamande Yehova.Tamandani Yehova.

  8. 1 Crônicas 5

    Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
    Capítulo 5
    Mostrando versículos 5–22 de 26

    5Mika,Reaya, Baala,

    12Mtsogoleri wawo ku Basani anali Yoweli, wachiwiri anali Safamu, kenaka Yanayi ndi Safati.

    22enanso ambiri anaphedwa, chifukwa nkhondoyo inali ya Mulungu. Ndipo iwo anakhala mʼdzikomo mpaka pa nthawi ya ukapolo.

  9. Lucas 2

    Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
    Capítulo 2
    Mostrando versículos 6–30 de 52

    6Ali kumeneko, nthawi inakwana yakuti mwana abadwe,

    11Lero mʼmudzi wa Davide wakubwadwirani Mpulumutsi; Iye ndi Khristu Ambuye.

    30Pakuti maso anga aona chipulumutso chanu,

  10. Salmos 84

    Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
    Capítulo 84
    Mostrando versículos 1–8 de 12

    1Malo anu okhalamo ndi okomadi,Inu Yehova Wamphamvuzonse!

    4Odala amene amakhala mʼNyumba yanu;nthawi zonse amakutamandani.Sela

    8Imvani pemphero langa, Inu Yehova Mulungu Wamphamvuzonse;mvereni Inu Mulungu wa Yakobo.Sela

  11. Salmos 62

    Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
    Capítulo 62
    Mostrando versículos 1–8 de 12

    1Moyo wanga umapeza mpumulo mwa Mulungu yekha;chipulumutso changa chimachokera kwa Iye.

    7Chipulumutso changa ndi ulemu wanga zimachokera kwa Mulungu:Iye ndiye thanthwe langa lamphamvu; Mulungu ndiye pothawira panga.

    8Dalirani Iye nthawi zonse, inu anthu;khuthulani mitima yanu kwa Iye,pakuti Mulungu ndiye pothawirapo pathu.Sela

  12. Salmos 85

    Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
    Capítulo 85
    Mostrando versículos 2–7 de 13

    2Munakhululukira mphulupulu za anthu anundi kuphimba machimo awo onse.Sela

    4Tibwezeretseninso mwakale Inu Mulungu Mpulumutsi wathu,ndipo mutichotsere mkwiyo wanu.

    7Tionetseni chikondi chanu chosatha, Inu Yehova,ndipo tipatseni chipulumutso chanu.

  13. Salmos 7

    Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
    Capítulo 7
    Mostrando versículos 6–10 de 17

    6Nyamukani Yehova, mu mkwiyo wanu;nyamukani kutsutsana ndi mkwiyo wa adani anga.Dzukani Mulungu wanga, lamulirani chilungamo chanu.

    7Lolani gulu la anthu a mitundu ina lisonkhane mokuzungulirani.Alamulireni muli kumwambako;

    10Chishango changa ndi Mulungu Wammwambamwamba,amene amapulumutsa olungama mtima.

  14. Salmos 74

    Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
    Capítulo 74
    Mostrando versículos 1–11 de 23

    1Nʼchifukwa chiyani mwatitaya ife kwamuyaya, Inu Mulungu?Chifukwa chiyani mkwiyo wanu ukutukutira pa nkhosa za busa lanu?

    3Tembenuzani mapazi kuloza ku mabwinja awa amuyayachiwonongeko ichi chonse mdani wabweretsa pa malo opatulika.

    11Chifukwa chiyani mukubweza dzanja lanu lamanja?Litulutseni kuchoka pachifuwa chanu ndipo muwawononge!

  15. Salmos 67

    Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
    Capítulo 67
    Mostrando versículos 1–6 de 7

    1Yehova atikomere mtima ndi kutidalitsa,achititse kuti nkhope yake itiwalire.

    2Kuti njira zanu zidziwike pa dziko lapansi,chipulumutso chanu pakati pa mitundu yonse.

    6Nthaka yabereka zokolola zake;tidalitseni Mulungu wathu.

  16. Salmos 28

    Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
    Capítulo 28
    Mostrando versículos 7–9 de 9

    7Yehova ndiye mphamvu yanga ndi chishango changa;mtima wanga umadalira Iye, ndipo Ine ndathandizidwa.Mtima wanga umalumphalumpha chifukwa cha chimwemwendipo ndidzayamika Iye mʼnyimbo.

    8Yehova ndi mphamvu ya anthu ake,linga la chipulumutso kwa wodzozedwa wake.

    9Pulumutsani anthu anu ndipo mudalitse cholowa chanu;mukhale mʼbusa wawo ndipo muwakweze kwamuyaya.

  17. Salmos 20

    Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
    Capítulo 20
    Mostrando versículos 1–9 de 9

    1Yehova akuyankhe pamene uli pa msautso;dzina la Mulungu wa Yakobo likuteteze.

    3Iye akumbukire nsembe zako zonsendipo alandire nsembe zako zopsereza.Sela

    9Inu Yehova, pulumutsani mfumu!Tiyankheni pamene tikuyitanani!

  18. Salmos 80

    Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
    Capítulo 80
    Mostrando versículos 2–19 de 19

    2kwa Efereimu, Benjamini ndi Manase.Utsani mphamvu yanu;bwerani ndi kutipulumutsa.

    15muzu umene dzanja lanu lamanja ladzala,mwana amene inu munamukuza nokha.

    19Tibwezereni mwakale Inu Yehova Mulungu Wamphamvuzonsenkhope yanu itiwalirekuti tipulumutsidwe.

Léxico (correspondência exata) Semântico (correspondência relacionada) Versículos omitidos Contexto do capítulo