Pular para o conteúdo
Publicidade

YESAYA 29

13 Ambuye akuti,

"Anthu awa amandipembedza Ine ndi pakamwa pawo,

ndi kundilemekeza Ine ndi milomo yawo,

koma mitima yawo ili kutali ndi Ine.

Kundipembedza kwawo ndi kwa chiphamaso.

Amandipembedza motsata malamulo a anthu amene anaphunzitsidwa.

Estes versículos te tocaram? Ore agora!

+581 estão orando agora.

Junte-se à corrente de oração.

Veja também