16 Inu mumazondotsa zinthu
ngati kuti dothi lasanduka wowumba mbiya.
Kodi chinthu chopangidwa chingawuze wochipanga kuti
"Sunandipange ndi iwe?"
Kapena mʼphika kunena kwa amene anawuwumba kuti,
"Iwe sudziwa chilichonse?"
16 Inu mumazondotsa zinthu
ngati kuti dothi lasanduka wowumba mbiya.
Kodi chinthu chopangidwa chingawuze wochipanga kuti
"Sunandipange ndi iwe?"
Kapena mʼphika kunena kwa amene anawuwumba kuti,
"Iwe sudziwa chilichonse?"