3 Mawu a wofuwula mʼchipululu akuti,
"Konzani njira ya Yehova
mʼchipululu;
wongolani njira zake;
msewu owongoka wa Mulungu wathu mʼdziko lopanda kanthu.
3 Mawu a wofuwula mʼchipululu akuti,
"Konzani njira ya Yehova
mʼchipululu;
wongolani njira zake;
msewu owongoka wa Mulungu wathu mʼdziko lopanda kanthu.
+581 estão orando agora.
Junte-se à corrente de oração.