Publicidade

Isaías 45

9 "Tsoka kwa wokangana ndi mlengi wake,

ngakhale kuti ali ngati phale chabe pakati pa mapale anzake.

Kodi dongo lingafunse munthu wowumba kuti,

Kodi ukuwumba chiyani?

Kodi ntchito yako inganene kuti,

Ulibe luso?

Veja também

Publicidade
Bíblia Online Bíblia Online

Bíblia Online • Versão: 2026-06-28_14-13-17-