Pular para o conteúdo
Publicidade

YESAYA 51

6 Kwezani maso anu mlengalenga,

yangʼanani pansi pa dziko;

mlengalenga udzazimirira ngati utsi,

dziko lapansi lidzatha ngati chovala

ndipo anthu ake adzafa ngati nsabwe.

Koma chipulumutso changa chidzakhala mpaka muyaya,

chilungamo changa chidzakhala cha nthawi zonse.

Estes versículos te tocaram? Ore agora!

+581 estão orando agora.

Junte-se à corrente de oração.

Veja também