Pular para o conteúdo
Publicidade

Isaías 53

12 Motero Ine ndidzamupatsa ulemu pamodzi ndi akuluakulu,

adzagawana zofunkha ndi ankhondo amphamvu,

popeza anapereka moyo wake mpaka kufa,

ndipo anamuyika mʼgulu la anthu olakwa kuti akhululukidwe.

Pakuti iye anasenza machimo a anthu ambiri,

ndipo anawapempherera anthu olakwa.

Veja também