Pular para o conteúdo
Publicidade

YESAYA 54

Ulemerero Wamʼtsogolo wa Ziyoni

1 "Sangalala, iwe mayi wosabala,

iwe amene sunabalepo mwana;

imba nyimbo, ndi kufuwula mwachimwemwe,

iwe amene sunamvepo ululu wa pobereka;

chifukwa mkazi wosiyidwa adzakhala ndi ana ambiri

kuposa mkazi wokwatiwa,"

akutero Yehova.

Estes versículos te tocaram? Ore agora!

+581 estão orando agora.

Junte-se à corrente de oração.

Veja também