Pular para o conteúdo
Publicidade

Isaías 54

Ulemerero Wamʼtsogolo wa Ziyoni

1 "Sangalala, iwe mayi wosabala,

iwe amene sunabalepo mwana;

imba nyimbo, ndi kufuwula mwachimwemwe,

iwe amene sunamvepo ululu wa pobereka;

chifukwa mkazi wosiyidwa adzakhala ndi ana ambiri

kuposa mkazi wokwatiwa,"

akutero Yehova.

Veja também