Pular para o conteúdo
Publicidade

Isaías 55

8 "Pakuti maganizo anga siwofanana ndi maganizo anu,

ngakhale njira zanu si njira zanga,"

akutero Yehova.

9 "Monga momwe mlengalenga muli kutali ndi dziko lapansi,

momwemonso zochita zanga nʼzolekana kutali ndi zochita zanu,

ndipo maganizo anga ndi osiyana kutali ndi maganizo anu.

Veja também