8 "Pakuti maganizo anga siwofanana ndi maganizo anu,
ngakhale njira zanu si njira zanga,"
akutero Yehova.
9 "Monga momwe mlengalenga muli kutali ndi dziko lapansi,
momwemonso zochita zanga nʼzolekana kutali ndi zochita zanu,
ndipo maganizo anga ndi osiyana kutali ndi maganizo anu.