9 Kodi Ine ndingangofikitsa amayi apakati mpaka nthawi yake yochira,
koma osalola kuti abaledi mwana?" akutero Yehova.
"Kodi ndingatseke mimba
pa nthawi yoti abeleke?" akutero Mulungu wako.
9 Kodi Ine ndingangofikitsa amayi apakati mpaka nthawi yake yochira,
koma osalola kuti abaledi mwana?" akutero Yehova.
"Kodi ndingatseke mimba
pa nthawi yoti abeleke?" akutero Mulungu wako.