Publicidade

Isaías 9

3 Inu mwauchulukitsa mtundu wanu

ndipo mwawonjezera chimwemwe chawo.

Iwo akukondwa pamaso panu,

ngati mmene anthu amakondwera nthawi yokolola,

ngatinso mmene anthu amakondwera

pamene akugawana zolanda ku nkhondo.

Veja também

Bíblia Online Bíblia Online

Bíblia Online • Versão: 2026-07-04_15-35-42-