4 Nambho ndhawi yeneyene yapo idakwana Amnungu adamtuma Mwana wao uyo pajhiko lino la panjhi. Mwana uyo wadabadwa ni wamkazi, mwana mmeneyo wadachgozedwa ni thauko la Musa, 5 waombole anyiwajha achogozedwa ni thauko, dala ife Ayahudi tichitidwe kukhala wana Amnungu.