Publicidade

Isaías 53

5 Koma iye analasidwa chifukwa cha zolakwa zathu,

ndipo anamuzunza chifukwa cha zoyipa zathu;

iye analangidwa kuti ife tikhale ndi mtendere,

ndipo ndi mabala ake ife tinachiritsidwa.

6 Ife tonse, ngati nkhosa, tasochera,

aliyense mwa ife akungodziyendera;

ndipo Yehova wamusenzetsa

zoyipa zathu zonse.

7 Anthu anamuzunza ndi kumusautsa,

koma sanayankhule kanthu.

Monga mwana wankhosa wopita naye kokamupha amachitira,

kapena monga nkhosa imakhalira duu poyimeta,

momwemonso iye sanatsekule pakamwa pake.

Veja também

Publicidade
Bíblia Online Bíblia Online

Bíblia Online • Versão: 2026-06-29_22-07-56-