Pular para o conteúdo
Publicidade

YESAYA 66

2 Kodi si manja anga amene anapanga zinthu zonsezi,

motero zonsezi ndi zanga?"

Akutero Yehova.

"Koma munthu amene ndimakondwera naye ndi uyu:

amene ali wodzichepetsa ndi wosweka mtima,

ndipo amamvera mawu anga.

Estes versículos te tocaram? Ore agora!

+581 estão orando agora.

Junte-se à corrente de oração.

Veja também