Kunyenyekela ni Ukulu wa Kilisito
1 Kukakhala ni chindhu chalichonjhe cha kukutilani mtima kwa kulunjidwa Nikilisito, kukakhala ni mtendele walionjhe wa chikondi. Kugwilizana ni Mzimu, lika khalapo lisungu ni kulekelela wina. 2 Chitani yajha siyakwaniliche chimwemwe changa, ili mukhale ni kugwilizana, chikondi chimojhi, mtima umojhi ni kuganizila pamojhi.