Pular para o conteúdo
Publicidade

Romanos 8

Kukhala kwa mbhavu za Mzimu wa Mnungu

1 Chipano palibe lamulo la chilango kwa anyiwajha yao muukhalo wao alunjana ni Kilisito. 2 Pakuti thauko la Mzimu ilo lipeleka umoyo kwa kulanjana ni kilisito Yesu, yanilekelela kuchokela mthauko la machimo ilo lipeleka nyifa. 3 Mnungu wadachita chindhu chijha thauko silidakhoze kuchita, ndande ya kuchepekela kwa Mundhu. Mnungu wadamtuma Mwana wake uku wali ni thupi ngati umo tili ife, dala wayachoche machimo kwa thupi lake, ni kwa thupi limwelo wayachoche machimo. 4 Mnungu wadachita chimwecho kuti tikhoze kuchita yajha yafunika ni thauko, kwa kumkhulupilila mzimu wa Mnungu pambuyo pa kuyavela makhumbilo ya matupi yathu.

Veja também