Pular para o conteúdo
Publicidade

Efésios 4

11 Nde uyo wapacha wandhu mbhaso za Mzimu wa Mnungu, wina kukhala atumwi, wina alosi wina olalikila Uthenga Wabwino, wina abusa ni wina oyaluza. 12 Adachita chimwecho ndande ya kwakonjekela wandhu wonjhe a Mnungu, kwa njhito ya kumtumikila Kilisito chimwecho okhulupilila onjhe akhala nganganga ngati umo lili thupi la Kilisito.

Veja também

Efésios
Ver todos os capítulos de Efésios