Pular para o conteúdo
Publicidade

Aloma 5

9 Pakuti saino tavomelezeka ni Mnungu kwa mwazi wa kilisito, chimwecho sitiomboledwe kuchokela mmbwayi yaikulu ya Mnungu! 10 Yapo tidali tikali adani a Mnungu, Mnungu wadachita ubwenji ni ife kwa njila ya nyifa ya mwana wake. Ndande chipano takhala abwenji wa Amnungu, ndiipo tikhoza kupheza uzene kuti Atate siatiombole kuchokela ku mbhwayi yake, pakuti Yesu ni umoyo masiku yonjhe. 11 Osati yameneyope, nambho tikondwela mkati mwa Amnungu kwa njila ya Ambuye wathu Yesu Kilisito, uyo wativanichana ni Mnungu.

Estes versículos te tocaram? Ore agora!

+581 estão orando agora.

Junte-se à corrente de oração.

Veja também