23 Anyiiwo ni atumiki a kilisito? Nikamba ngati wamsala, ine ni mtumiki wa Kilisito kupitilila anyiiwo. Nachita njhito yolimba kupunda, namangidwa mndende mala zambili, nabulidwa mikwapulo kupunda, nawandikilidwa ni nyifa kupitilila anyiiwo. 24 Mala kasano nabulidwa mikwapulo, nikila yapo nimabulidwa, nimabulidwa mikwapulo selasina ni tisa ni Ayahudi. 25 Nida tyapidwa katatu ni Alumi nidabulidwa myala kamojhi, sitima yaniwanangikila katatu mnyanja nchele, nidakhala chonga mmajhi usiku usana. 26 Mmaulendo mala zambili nazengedwa ni mafuliko ya majhi, nidavutika kwa kubulidwa ni anghungu, nidavutika kuchokela kwa wandhu ajhiko langa, nidavutika kuchokela kwa wandhu amaiko ina, nidavutika mmijhini, nidavutika mmatengo, nidavutika mnyanja nchele, nidavutika kuchokela kwa achabale aunami. 27 Nachita njhito ni kulaga, nachezelela mala zambili, nakhala ni njala ni lujho mala zambili, nidakosa chakudya mala zambili ni kukhala mozizila popande njhalu. 28 Kupitilila yameneyo yonjhe, siku zonjhe niganizila nghani za magulu yonjhe ya wandhu amkhulupilila Yesu.
Publicidade
2 Coríntios 11
Estes versículos te tocaram? Ore agora!
+581 estão orando agora.
Junte-se à corrente de oração.