Pular para o conteúdo
Publicidade

Resultados da busca por "salvação"

45 resultados encontrados

  1. João 20

    Nyanja
    Capítulo 20
    Mostrando versículos 7–10 de 31

    7ni chitambaa icho wadamangidwa Yesu kumutu. Sichidaikidwe pamojhi ni sanda, nambho chavilingidwa ni kuikidwa pachokha.

    8Ndiipo oyaluzidwa mwina uyo wadachoghola pa chiliza, wadalowa mkati wadaona ni kukhulupilila.

    10Chimwecho oyaluzidwa adabwela kukhomo.

  2. Marcos 8

    Nyanja
    Capítulo 8
    Mostrando versículos 5–37 de 38

    5Yesu wadaafunjha, "Muli ni mabumunda yangati?" Adamuyangha, "Tili ni mabumunda saba."

    36Bwanji, mundhu siwapate phindu lanji wakavipata vindhu vonjhe vapajhiko, nambho wakautaiza umoyo wake?

    37Mundhu siwachoche chiyani kuti wakhoze kuombola umoyo wake?

  3. 2 Coríntios 3

    Nyanja
    Capítulo 3
    Mostrando versículos 4–12 de 18

    4Uku nde kupilila uko tilinako pamaso pa Mnungu kwa kupitila yajha wadayachita Kilisito.

    8utumiki wa Mzimu wa Mnungu ukhala ni ulemelelo waukulu kupunda.

    12Tili ni kulimba mtima kupunda pakuti tili ni chikhulupililo cha mtundu uwu.

  4. 1 Coríntios 1

    Nyanja
    Capítulo 1
    Mostrando versículos 5–29 de 31

    5Pa kulunjana ni Kilisito mwakhala ni mwayi kwa kila kandhu, yaani pakukamba konjhe ni njelu.

    6Uthenga wa Kilisito uwo mudakambidwa ni wauzene,

    29Ichi mateyake wali ni thupi waliyonjhe siwadajhi elekela pachogolo pa Mnungu.

  5. Efésios 5

    Nyanja
    Capítulo 5
    Mostrando versículos 13–29 de 33

    13Nambho chilichonjhe icho chavumbula ni dangalila, sichioneke,

    14ndande chilichonjhe icho chavumbulidwa, chikhala dangalila. Nde ndande yalembedwa Mumalembo ya Mnungu,"Uka iwe waghona,uhyuke,Kilisito siwakuwalichile dangalila lake."

    29Palibe mundhu uyo waliipila thupi lake, nambho walidyecha ni kuliveka. Nde umo Kilisito walisungila gulu lake,

  6. João 10

    Nyanja
    Capítulo 10
    Mostrando versículos 2–39 de 42

    2Nambho uyo walowa koopitila chicheko chimecho, mmeneyo nde owesa wa mbelele.

    28Ine napacha umoyo wamuyaya ni muyaya siasiana ni Amnungu.

    39Adaesanjho kumgwila nambho wadapulumuka mmanja mwao.

  7. 1 Coríntios 10

    Nyanja
    Capítulo 10
    Mostrando versículos 4–19 de 33

    4ni wonjhe adamwa chakumwa chinchijha chidacho kwa Mnungu. Adamwa kuchoka mujha mumwala waukulu wa uzimu uwo udachata, ni mwala waukulu umeneo udali Kilisito mwene wake.

    17Pakuti bumunda nilimojhi, ife taonjhe tili ambili tili thupi limojhi, taonjhe tililandila bumunda limwelo limojhi.

    19Chipano, nikambe chiyani, kuti chijha chachochedwa njhembe kwa viboliboli ni chindhu?

  8. Filipenses 3

    Nyanja
    Capítulo 3
    Mostrando versículos 8–16 de 21

    8Kupitilila yameneyo niwelenga vindhu vimenevo sinipata nikailinganicha ni kupata lalikulu lipitilila mwa pakumjhiwa Kilisito Yesu Ambuye wanga. Ndande yake navomela kusiya kila kandhu nayaona yalibe mate ili nimpate Muomboli

    9nane nilunjane nayo. Nisidajhi vomela namwene kwa kuchata thauko ila ijha ipezeka kwa chikhulupi mwa Kilisito kuvoleka kuchokela kwa Mnungu kwa chikhulupi.

    16Nambho tilisunge kupunda lijha tauko likwanilicha.

  9. Lucas 5

    Nyanja
    Capítulo 5
    Mostrando versículos 17–28 de 39

    17Siku limojhi Yesuyapo wamayaluza wandhu, Afalisayo ni oyaluza a mathauko kuchokela kumijhi yonjhe ya Yudea ni Galilaya, ni Yelusalemu adajha pamwepo. Ni mbhamvu za Ambuye zidali ni iye kuti walamiche odwala.

    23Chiti icho chili lahisi kupunda, kukamba, ‘Walekeleledwa machimo yako.’ Kapina kukamba, ‘Ima ujhiyenda?’

    28Lawi wadanyakuka ni wadasiya yonjhe nikumchata Yesu.

  10. 2 Coríntios 5

    Nyanja
    Capítulo 5
    Mostrando versículos 2–17 de 21

    2Chipano, tibuula kupunda yapo tikhala pajhiko nitipenyelela kwa khumbilo lalikulu kuvekedwa thupi la kumwamba.

    9Chimwecho chindhu chachikulu kupunda ni kumkwadilicha, ikhale tikhala pano pajhiko kapina kumeneko kumwamba.

    17Chimwecho mundhu waliyonjhe wakalunjana ni Kilisito, wakhala mundhu wa chipano, yakale yatha, yakhala yachipano.

  11. Efésios 4

    Nyanja
    Capítulo 4
    Mostrando versículos 10–27 de 32

    10Chipano mmeneyo uyo wachika nde uyo wadakwela kumwamba kupunda, dala waenele kila pamalo.

    16Kwa kuchogozedwa ni Kilisito, thupi lonjhe likalunjidwa ni kugwilizidwa pamojhi, kwa mthandizo wa kila chiwalo. Chipano, kila chiwalo chichita njhito yake, thupi lonjhe likula lene ni kujhikonja muchikondi.

    27dala simudampacha Satana malo.

  12. Atos 3

    Nyanja
    Capítulo 3
    Mostrando versículos 5–23 de 26

    5Mundhu yujha wadaapenya niwalindilila kupata kandhu kuchokela kwa anyiiwo.

    21uyo wamafunika kulandilidwa kumwamba mbaka ijhe ndhawi yochita kila kandhu chikhale cha chipano. Nghani izi zimakambidwa ni Mnungu kupitila alosi wake woyela kuyambila chiyambo cha jhiko la panjhi.

    23Mundhu waliyonjhe uyo siwamuvela mlosi mmeneyo, siwapatulidwe kuchokela kwa wandhu a Mnungu ni kuphedwa.’

  13. Lucas 24

    Nyanja
    Capítulo 24
    Mostrando versículos 22–51 de 53

    22Ni wachikazi wina pagulu lathu atizizwicha. Adapita pachiliza lelo umawamawa,

    42Adampacha chibandhu cha njhomba yowamba.

    51Yesu yapo wamapacha mwawi, wadatengedwa kumwamba ni kwasiya ni kupita kumwamba.

  14. Romanos 6

    Nyanja
    Capítulo 6
    Mostrando versículos 8–18 de 23

    8Chipano, tamwalila pamojhi ni Kilisito, tikhulupilila kuti sitikhale pamojhi niiye.

    9Chipano tijhiwa Kilisito watohyukichidwa siwamwalilanjho ni nyifa simlamulanjho.

    18Mdaomboledwa kuchokela kuukapolo wa machimo, chipano mwakhala akapolo akuchita yajha yamkwadilicha Mnungu.

  15. Atos 8

    Nyanja
    Capítulo 8
    Mostrando versículos 1–7 de 40

    1Chinchijha, Saulo wadakondwelechedwa ni kujha kuphedwa kwa Sitefano.Kuyambila siku lijha wandhu adamkhulupilila Kilisito kujha ku Yelusalemu adayamba kuvutika kupunda. Wandhu wonjhe yawo adamkhulupilila Kilisito, kusiya atumwi, adamwazika ku malo yonjhe ya Yudea ni Samaliya.

    3Ndhawi imeneyo Saulo wamatowavuticha wandhu yawo adamkhulupilila Kilisito. Wadapita kila nyumba niwaakwekweta wandhu yawo adamkhulupilila Kilisito, wachikazi ni wachimuna ni kwaaika mundende.

    7Viwanda vidaachoka wandhu kwa kukweza mvekelo waukulu, wandhu wopuwala ni wovuwala adalamichidwa.

  16. Marcos 14

    Nyanja
    Capítulo 14
    Mostrando versículos 16–64 de 72

    16Oyaluzidwa adachoka, adapita kumujhi, adampeza kila chindhu chili ngati umo adakambilidwa ni Yesu. Adakonjekela chakudya cha Pasaka.

    42Nyakukani! Tijhipita! Mundhu uyo siwaning’anamuke wali pampano."

    64Mwachinawene mwavela umo wamkafulila Mnungu" Anyiimwe muona bwanji? Bwalo lonjhe lidamlamula waphedwe.

  17. Mateus 26

    Nyanja
    Capítulo 26
    Mostrando versículos 10–68 de 75

    10Yesu wadajhiwa icho amakamba, wadaakambila, "Ndande yanji mumchaucha wamkaziyu? Uyu wamkazi wanichitila chindhu chabwino kupunda.

    46Imani tijhipita. Yujha waning’anamuka watokujha."

    68adakamba, "Iwe Kilisito, tilosele! Yani uyo wakubula?"

  18. Romanos 8

    Nyanja
    Capítulo 8
    Mostrando versículos 34–39 de 39

    34Niyani uyo siwalamule kwa kwalanga? Palibe! Pakuti Kilisito nde uyo wadamwalila, ni wadahyuka ni wakhala kumalo ya ulamulilo kwa Mnungu iye watipembhela.

    35Niyani wakhoza kutiika patali nichikondi cha Kilisito? Bwanji ni kulaga, kapina mavuto, kapina njala, kapina kutedwa njhalu, kapina kuofyedwa kuphedwa?

    39kapina jhiko la kumwamba kapina jhiko la panjhi kupunda. Palibe choumbidwa chalichonjhe chikhoza kutiika patali ni chikondi cha Mnungu mkati mwa Kilisito Yesu mbuye wathu.

  19. Gálatas 6

    Nyanja
    Capítulo 6
    Mostrando versículos 2–15 de 18

    2Mthangatilane anyiimwe kwa anyiimwe kwakuchita chimwecho simkwanilichwe thauko la Kilisito.

    7Simdanyengeka, Amnungu sachitidwa chipongwe. Icho wavyala mundhu nde icho siwakolole

    15Kuchitidwa mdulidwe kapina kosachitidwe mdulidwe asati chindhu chamate, chamate ni kukhala choumbidwa cha chipano.

  20. Filipenses 2

    Nyanja
    Capítulo 2
    Mostrando versículos 5–9 de 30

    5Mukhale chimchijha ngati mujha muda khalilala ni Kilisito Yesu.

    8Wadanyenyekela ni kuvomela kumwalilanyifa ya pamtanda.

    9Ndande imeneyo Mnungu adamwika pamwamba kupundanikumpacha jhina lalikulu kupitilila kila jhina.

Léxico (correspondência exata) Semântico (correspondência relacionada) Versículos omitidos Contexto do capítulo