Pular para o conteúdo
Publicidade

Aloma 3

Kuvomelezedwa kwa njila ya kukhulupilila

21 Nambho chipano njila ya kwachita wandhu avomelezeke kwa Mnungu ili padanga, popande kukhulupilila thauko, osati ngati umo lidakambila thauko la Musa ni malembo ya alosi a Mnungu vonjhe vikambilila chindhu chimenecho. 22 Mnungu waavomela wandhu kuti ni woyela kwa njila ya chikhulupi chao kwa Yesu Kilisito, Mnungu wachita chimwecho kwa wonjhe akhulupilila, siwapatula Ayahudi ni wandhu yawo osati Ayahudi.

Veja também