4 Uku nde kupilila uko tilinako pamaso pa Mnungu kwa kupitila yajha wadayachita Kilisito. 5 Ife sitikhoza kalikonjhe kwa mbhavu zathu tachinawefe, nambho mbhavu zathu zichoka kwa Mnungu. 6 Iye nde uyo watikhozecha ife kukhala wotumikila pangano la chipano ilo osati pangano la thauko ilo lilembedwa, nambho pangano la Mzimu wa Mnungu. Pakuti thauko lalembedwa lipeleka nyifa, nambho Mzimu wa Mnungu upeleka umoyo.