Pular para o conteúdo
Publicidade

Vichito 2

Kujha kwa Mzimu Woyela

1 Yapo lidafika siku la pwando la Pentekosite, wandhu wonjhe yawo adamkhulupilila Yesu adasonghana malo yamojhi. 4 Wandhu wonjhe adajhazidwa ni Mzimu Woyela, adayamba kukamba mikambo ya chilendo, ngati umo wadafunila Mzimu Woyela.

Veja também