Pular para o conteúdo
Publicidade

Atos 2

17 Ambuye Amnungu akamba, Pa masiku yothela,

sinapache wandhu wonjhe Mzimu wanga.

Wana wanu ni anamwali wanu sialosele,

anyamata wanu saone maloso,

azee wanu saalote maloto.

18 Yetu ata mbowa zanga waachimuna ni waachikazi,

sinapache Mzimu wanga pa masiku yameneyo,

anyiiwo siachoche ulosi.

19 Sinichite vodabwicha kumwamba

ni vodabwicha pajhiko la panjihi.

Sikukhale mwazi, moto ni uchi waukulu.

20 Jhuwa silikhale mdima,

mwezi siukhale wofiwila ngati mwazi,

likali osafika siku lijha lalikulu ni laulemelelo la Ambuye.

21 Nambho, waliyonjhe uyo siwapembhele kwa jhina la Ambuye siwaomboledwe."

Veja também