17Bwanji, simujhiwa kuti chilichonjhe icho chilowa mkamwa chipitilila mmimba ni mathelo yake chipita kudambo?
18Nambho chindhu icho chituluka mkamwa chichoka mumtima, chimenecho nde icho chimchita mundhu siwadavomelezeka pakumlambila Mnungu.
29Yesu wadachokapo pa malo yajha ni kupita mbhepete mwa nyanja ya Galilaya. Wadakwela kuphili ni kukhala panjhi.