Pular para o conteúdo
Publicidade

Marcos 13

Mwana wa Mundhu siwajhe

24 "Ndiipo, siku zimenezo, yapo siyathe mavuto yameneyo, jhuwa silikhale mdima ni mwezi siuchocha dangalila. 25 Ndhondwa sizigwe kuchokela kumlengalenga, ni vindhu ivo vili kumlengalenga sivitingizidwe. 26 Pamenepo wandhu sianione ine Mwana wa Mundhu, ninijha nili mmitambo kwa mbhavu zambili ni ulemelelo. 27 Ndiipo sinaatume atumiki akumwamba wakuse wandhu wanga nidaasangha kuchokela kumadela yonjhe yanayi ya jhiko, kuchokela mmathelo ya jhiko, mbaka mmathelo ya kumwamba."

Veja também